Email a copy of '‘Ntopwa 1' not wanted man: Police say no arrest for DPP roughneck' to a friend
Loading ...
Email a copy of '‘Ntopwa 1' not wanted man: Police say no arrest for DPP roughneck' to a friend
Police in Rumphi have arrested Edwin Mtegha, 32, for allegedly defiling a 15-year-old mentally- challenged girl. Rumphi Police Station spokesperson...
Yalakwa apa police. Kuli konse ngakhale ku America social media ndi evidence ndithu. Anthu achikuda amaphedwa ndi apolisi ku States evidence yake social media. Interpol investigations za terrorism ya isis evidence yake social media. Azimayi kukozelana mkamwa ku area 24 evidence yake social media. Inunkhe lero social media chifukwa yajambula mtopwa 1. Musachulutse mantha, gwirani ntchito yanu kamumangeni. Osaopa che Mchacha
Typical of DWIPHWISI DEMOCRATIC PARTY
Sorry comrades citizens all three new IGs are very sick ,The have been tested to be HIV +++++++++ extra +,so no wonder their mentality is that way.
police can not arrest this fat pig, which cell are they going to put him.? There no cells for pigs in Malawi. Chimimba uko, munthu opanda nzeru.. His acts being endorsed by Mutharika himself, so you should know what a nutty professor he is.
DPP ndiyofoila, nthawi yawo yatha. Imagine Mchacha abusing Patricia Kaliati while the President is listening. If there was any form of leadership in DPP what Mchacha said would have been condemned right away. But the big man is busy sleeping on the job.
Useless police….
Police u are so stupid. Why did u arrest Kabwira, Chakhwantha and friends based on WhatsApp evidence? Why those Area 24 ladies were arrested based on social media evidence also? Why shielding these thugs? This is the reason why Jose will not be confirmed to be the IG.
a police ndinu zitsiru. nanga bwa jessy kabwila munamumanga coz of social media circulations. Ramsy Mshani ndiwe chitsiru chachitumbuka
DIPWIPWI WE SEE YOU AND WE KNOW YOU.YOUR DAYS ARE NUMBERED.Ana amulungu sangale kulira masiku onse amoyo wawo.#Mabalayomweija.
Ng’oma ikalila kwambiri sichedwa kung’ambika soon mudzava za awa adzafa ifa yowawa awa rumours said ndiomwe anapha mwana uja wa school and mene imaonekela video’yo amaphadi awa ndithuuu and adakaphaso apa… pano muli pa 39 next ndi 40 tikukuonanituuuu…. Chilima tiomboleeeeee Njoka sitiwetadi ndithu