Email a copy of 'Of Malawi reforms and the Chimwemwe Banda’s of this nation' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

54 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
mpipuimimi
mpipuimimi
9 years ago

chimwemwme can be dull but atleast she knows some job she is rewarded for. Inusno ngati muntha pitani mukawapeze mabwana mukawapange imene chimwemwe amawapanga ndiponso akupatsani anu ma udindo mavacancy ndi ambili; press officer ndi na otelowo. Bwanji kukokelana pansi. ngati chimwemwe ali ophweka kuti amavulira aliyense pitani mukayense mwayi tione ngati simukaomba khoma

uyuni
uyuni
9 years ago

if there has been a PS who is understanding, intelligent at information it is Chimwemwe. musachite nsanje munthu alibwino uyu

chatonda
chatonda
9 years ago

Chimwemwe got a surprise promotion to the position of Ps by Mr Wille Samute who is her long time sweet heart and this started when cHIMWEMWE was at Local government where Samute was Ps too. Get rid of Chimwemwe Banda for the benefit of the nation.

konzs
konzs
9 years ago
Reply to  chatonda

Zazii that’s her personal life Pangani zanu

Katakwe pa ndale
Katakwe pa ndale
9 years ago

If you have a problem wit dancing, don’t blame the tune

Kaka
Kaka
9 years ago

Incompetent and unproductive Chimwemwe Banda……. With this background i don’t expect u to work professionaly rather than ur cheap politics. Hatred will not take u anywhere and please don’t spoil MBC! Munthu wamkulu ngati iwe sungamakhale busy mu ofc mwako ndi kumasokoneza tsogolo la ana with a sound educational background and skillful. Asiye ana agwire ntchito yawo bwinobwino osati kuwazunza lyk this. Only time will tell, zako zikutsata ndipo udzalira ndi kukukuta mano…… Free advice!!

chakwanuleka
chakwanuleka
9 years ago

Chimwemwe read the articles with a sober mind and wear a human face. Remember what we used to say that ukakhala pa nsana was njobvu usamati kulibe mame. Chifukwa tsiku lina mudzatsika pa nsana was DPP ndiye anthu mukuponderezawa mudzawafuna. What you sow you also reap

obaba
obaba
9 years ago
Reply to  chakwanuleka

mmmmm

Dzeya
Dzeya
9 years ago

so how many controller of news does mbc have? 4 – radio 2 and tv 2? and with 10 or 11 directors ( acting and redeployed but still on mbc payroll) mmmmm how big is mbc?

MBACHI
MBACHI
9 years ago

NAPEPE AKUMPOTO. NO CHANCE.

MBACHI
MBACHI
9 years ago

It is a fact that this reform you want your relatives and Tcholo people to dominate.

powder
powder
9 years ago

adakuuzani kuti enao adzakhalapo kwa muyaya? mesa enanso akufuna maudindo? adikire enawo adzamwalire? mesa ophunzira onse amafuna kugwira ntchito yomwe adaphunzira kuonetsa luso lawo, tingokhalira za amodzimodzi? zanunso izo, zasinthabe

Read previous post:
Waiting upon the Lord

Waiting upon the Lord can transform us into a people of growing faith. The word wait means to hope, to...

Close