Email a copy of 'On Kamuzu Day and some May 21 political balderdash' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'On Kamuzu Day and some May 21 political balderdash' to a friend
United Democratic Front (UDF) presidential candidate Atupele Muluzi has said that politics is a service to the people politicians serve. Speaking at...
Kamuzu was great period!!!
What ever, kamuzu was a great leader,he was not a crook, at least he was honest to the country’s money. Now what Malawi needs is somebody like kamuzu banda or imran khan come to rescue Malawi,
Surely speaking it’s only Dr Lazarus Chakwera who can revitalize Kamuzu legacy and Malawi can be on track why it’s because of thefour corner stoneUNITY LAYALTY OBEDIENCE AND DESCIPLINE Kamuzu maneged to lead the nation and built patriotism in youth week self help spirit
At least nyasa mwabweletsa munthu amene walemba zokhudzana ndi tsiku la lero, musamayese zida,anthu tikuona zomwe zikuchitika,palibenso kuvotera kuti uyu ndiwakwathu,ayi,tikufuna development oriented leader.
OMG ..Iyi ndi misala. Power hungry ! Munthu u President akuwufuna uyu. No family members basi iye ndi achipani chake. Court contempt
It is not people, it is about leadership and putting systems to work. UDF, MCP, PP DPP has not done that, we of UTM will do that. Simple
SURE UTM FIRE KUTI BUUUUUUUUU!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!
vuto lomwe lilipo ndilakuti a Malawi sititha kuonapo zabwino zomwe munthu wachitapo koma kungokhala negative pa chilichonse basi.Kodi kaganizidwe ka chonchoko tingatukule dziko?Mu nthawi ya Dr.Banda panali zolakwika ndithu koma zambiri zinali zabwino chifukwa dziko lino Kamuzu analipeza lilibe mseu olo umodzi wa phula,zipatala kunalibeko ,maphunziro kunalibeko,airport yowoneka bwino kunalibeko,mwachidule he started from the scratch.Come Bakili Muluzi,his speeches throughout attacking Kamuzu portraying kamuzu ngati sanapange chilichonse.Mu dziko muno manadzalidwa mbewu yosaona zabwino koma zoipa zokhazokha .Zotsatira za izi ndi mzimu wosakhululukirana komanso mzimu wosayamikirana.Amalawi tiyeni tisinthe moyo uwu chifukwa tikapanda kutero Mulungu sadalitse dziko lathu.Tiphunzire kukondana posatengera zigawo chifukwa malawi… Read more »