Email a copy of ''Opposition from hell’ Minister Chiumia accuses MCP, Chakwera of confrotation' to a friend
Loading ...
Email a copy of ''Opposition from hell’ Minister Chiumia accuses MCP, Chakwera of confrotation' to a friend
First Merchant Bank (FMB) staff members are bitterly complaining over racist attacks on fellow members of staff especially from credit department...
Indeed, What has dpp government done with advice from The Late Robson Chirwa? (May his soul rest in peace) Anthu nkumakunena iweyo honourable? What a waste of honour!
@Zabweka. We could do with logical contributions, not kutukwana.
DPP ndiyamwano kwambiri ndipo sikumva upangiri wina ulionse.chaka chatha Chakwera adapereka nzeru,Inu mmalo motenga nzeruzo mudatuma mafumu kumakatukwana Chakwera,Pa Christmas ngati si pa new year adakuuzani upangiri Inu mudachita mwano,posachedwapa akuuzani otsutsa Inu mutuma mafumu kumakayakha zamwano ndiye anduna mufuna munene chiyani? Kodi mitu yanu sikugwira ku bomako eti.Muziganiza zotukula aMalawi osati chipani,vuto lanu mumakhala buze ndikuba ndalama zochitira kampeni.Mulungu akuona zonse ndipo tsikulina mudzabwezera zonse mudaba.
Bravo Gilly asamakudele anyani awa
Mose I we mwalemba apa vindele pela chi end Rift Valley ukununkha na pa intone suwon
The Lady is intelligent Bravo Obama always inspiring me Receive Showers of blessings
Let us get this clear. MCP has no control over Reserve Bank, ACB, Ministry of Finance, Directorate of Public Procurement, Asset Declaration, etc etc. Briefly put, MCP is not in control of government affairs. MCP and other opposition parties can only point out wrongs, maladministration, or advise when things are going wrong. It has done so during Parliament sittings, especially when discussing the budget. The opposition moved a motion to make ACB independent in line with DPP manifesto. We know what rôle economically an independent ACB would play. Now, honourable minister, can you please elaborate on how MCP has contributed… Read more »
Ine koma Grace chiumia! Ishiiiii amangondinyasa basi ndipo pa screen panga sindifuna kumuwona. I don’t know ngati nyasi zimenezi zinakwatiwapo.
Chakwera ndi mwana wandani? ali ndi mzeru zanji?
Anatsiya nkhosa zikutsochera,iye kuthamangira ndalama ku ndale, nde angatsogolere mtundu wa amalawi?
Ndiwakuba uyu!
Yemwe akuti dziko silikuyenda bwino akufuna liziyendetsedwa motani? Adzipatsidwa ndalama atsagwire ntchito?
Koma iwe,iwe chakwera mbuzi unditsamale!!
This minister needs a sandpaper to smoothen her face, no wonder this is affecting her brain and thinking capacity