Email a copy of 'Pastor Salanje admits being rude: ‘I don’t need Malawians, they are calling me Satanic’' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Pastor Salanje admits being rude: ‘I don’t need Malawians, they are calling me Satanic’' to a friend
The World Bank office in Malawi has rejected accusations by some Civil Society Organisation (CSOs) that the institution was dictating...
Mr u going no way in RSA,unfortunetely you in the wrong place…procced
Salanje akunena zoona a Malawi ife tili ndi nsanje .Sitifuna kuona mzathu akutukuka tidakali ndi maganizo akuti amaene angalemele ndi auje .Pamene Mulungu polenga
aliyense anampatsa mwai wake tifune olo tisafune ngati Mulungu anati udzakhala
chonchi ndiye kuti udzakhala chonchi komanso tidzikhala ndi ambition Mulungunso
amathandiza munthu wodzithandiza yekha.
The judgment z around the corner.
Inu a Salanje mukuonekeratu kuti muli pa mavuto a akulu, chuma muli nacho koma sichinga gule mtendere pongonena kuti simudzabweranso ku Malawi zikusonyeza kusowa mtendere ndi po tchubula za magalimoto zikusonyeza kuti munali ndi mangaw ndi anthu ena ndiye mukufuna muwauze kuti or mudane nane ndapambabe. Akazi anu ndi ana anu akanakhala anzeru bwenzi akuti amuna anga kapena a bambo musatero si bwino. Taonani matama anuwo mwalandira nao nyozo ulemu wonse kuchokeratu ndi anthu amene samakuziwani kuti munapezeka ndi ziwaro za anthu mu fridge akudziwa. Mashoni siyinkhala ndi mpanda wotero ku Joni musatinamize. Ndimmene mwaonera nokha ndemanga za a Malawi… Read more »
Za pa dziko nzachabe chabe anatero Mlaliki (Ecclesiastic)
CHUMA CHOPEZA UTAKALAMBA CHIMAZUNGUZADI MUTU ETI????????????????????????????
hahahahahaaaa mr Salanje sopano pitanidi ku America ifenso kuno sitikukufunani musazabwelenso,M’busa kunyanyala Nkhosa zomwe mbuye wake wamupasa kuti azisamale zoona???
Signs of the times.
zaziii!! osawathandiza abale anu ku Ntcheu ku Chinkhwamba akuchita kusowa nyumba aja bwanji? which god z this??
Pastor of sineers salanje