Email a copy of 'Police arrest DPP councillor, chief over stolen LDF items in Zomba' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Police arrest DPP councillor, chief over stolen LDF items in Zomba' to a friend
What started as a simple exercise to harness honey inside Nyungwe Catholic Church in Chiradzulu on Sunday night has led...
Councillor ameneyo ndiwochitisa manyazi zedi.Komwe umalandira sikokwanira?Chisiru!!!!!
This is what most DPP councillors are doing. Akuti boma ndi lawo choncho angathe kuchita chili chonse kuphatikiza kuba. This is just one of the many ugly scenarios. Nanga a Mulhako mulinso ndi mawu apa? Si wanuyi wakuvulani basi! Anawatu akuonera. Shame! Yatsala ya K92 bn ija. MBAVA!!!
Mwabisa zambiri tell us more
Galu was DPP ameneyu awzolowera cashgate zachamba basis isi!!,
Now this is the Malawi I know, there’s no way someone is simply a thief if he is in govt, and where the reporter has not given you any indication as to what the thief’s motives are we rush to attach it to the party.
Any man is ruled by self preservation, and thieving is just a manifestation of self preservation. It is only a matter of how far YOU as an individual are willing to go. Let the law deal with these clowns accordingly. And then we might have a better chance to weigh this moment in our history.
Tsiku lina ndinalota nyumba yosanjikizana itagwa ndipo aliyense ofika pamalopo analira.
That’s what people are paying for their crave of voting for party colours and symbols.
Nkhuku imatenga make unyera mnyumba
Alomwe akubera alomwe anzawo aku Ntonya paja Bingu adaberanso alomwe ,Pitara ndi mkazi wache adaba ndalama zama ARVS pano Councillor wachilomwe wabera Anophiya anzake kikikikiki kumbwambwana si uku?umve ku Dpp
Amaona kuchedwa