Email a copy of 'Police arrest Lilongwe head teacher for embezzling MSCE exams fees' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Police arrest Lilongwe head teacher for embezzling MSCE exams fees' to a friend
As countdown to Standard Bank “Be More" Lilongwe race scheduled for July 30, 2017 continues, Standard Bank has dared prospective...
Zonvesa chisoni kuwatero ana. Ndye akufuna ana atani amene nthawi imeneyi please a maneb chitanipo kanthu mwa changu
A phunzitsi amenewo. Sanadziwe kuti akhoza kumanga. Mwina anangidzimwera mowa ameneyo. Koma ndalama take ndiyochepa kwambiri angapange NATO chiyani imeneyi. Be rensiposible, sir. Mwawona mukalo Nazi Ku ndende za zii. Komanso wawononga tsogolo la ana.
Makolo awo amaganiza kuti athana nayo budget ya fizi, iye kuwabwenzela mumbuyo.
Kuzunza ana uku,kuvutika kuwerenga, kupereka fees wina kungowadyera. Chilango choyenera ndiye kumulamulo kuti atenge responsibility ya ana 19 wo powalipilira tuition,transport,lunch ndi examination fees mpaka adzalembe next exam. Mfiti ya munthu! kuzolowera nyau basi,usandilankhulitse pambali mwana wa Chimbano chidzukulu cha Kangw’ingwi.
ochewa