Email a copy of 'Political scientist tells CSOs to challenge DPP on counter demo' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Political scientist tells CSOs to challenge DPP on counter demo' to a friend
State rights body, the Malawi Human Rights Commission (MHRC) has launched an investigation into the petrol bombing of vocal civil...
It will be a useless Demo.Angofuna azimusokoneza President ogwira ntchito uyu.The Goodness with Peter Mutharika is that he concentrates on his job other than playing like what VP is doing just wasting tax payers money busy campaigning for his UTM.
Kupanga ma demo si bvuto. Bvuto ndi a pumbwa amene amafuna kusokoneza. Ma demo limakha liu la amalawi onse okhudzidwa mdziko. So go ahead with demo
Much as I do not agree with mchacha and his cadets whose reign ends on 21 may 2019, I also don’t agree with the holding of demonstrations to force the president to resign. No matter what happens I don’t see the president resigning from his post. CSOs should just go and campaign hard so that people do not vote for DPP and muthalika. U mean if Peter resigns then chilima takes over as president? This is childish! Am not a member of DPP but MCP and my vote is for chakwera. Mtambo go back to drawing board.
A Mtambo a chitsiru awa. Asowa chokanena kwa ma donor amene amawabera ndalamazo. Mchacha wachita bwino. Zizete za ma CSO zizikapanga ma demo awowo mtchire ife a DPP tilkulimbikitsa chitukuko cha miseu muno mMalawi. Mmalo molimbikitsa kukonza miseu ndiye wina azisokoneza nkumayendamo ndawala zopanda pake? Mukafune kochita manyi anuwo osati mmiseu yomwe tikukonza ife.
Owen Khamula is at it again. My brother get your facts straight there’s no way that DPP can be shaken by UTM in Mulanje, Thyolo and Chiradzulu. Dude ngati ukudya za UTM sibwino kuti uzidya za ulele, auze chilungamo a utm kuti alibe chance ku maboma amenewo.
I disagree with Mr Thindwa, the CSOs have done well Dpp is the party of violence.
The country is slowly turning into a dictator
This is the country we fought for
life is becoming unbearable
we are slowly becoming endocrinated .
Regionalised, Tribalised finally bred hatred.
The policies we make are nolonger national but regional
All state funded institions have been turned into party institutions.
Check the status of admarc MBC water board, Escom leave alot to be desired
we nolonger postively comments, our comments reflect how rotten we have become
poor Country.
DPP ikupangitsa manyazi a Lohmwe tonse. Mchacha is terrorist on one.
Wabodza iwe si mulhomwe James. Mulhomwe salankhula zopusa ngati zakozo.
Kutsutsa zomwe James akunena nde ulhomwewo umenewo
Mayina aketu akumakhala Thindwa, Mtembo, Makhumbo Munthali, etc……WAKWITHU SUPPORT SYNDROME. This is not national interest but tribal. It’s a fight between the Tumbukas and the Lhomwes and they want to involve the whole country in their tribal wars and pursuits. That’s not fair.
Koma Mtumbuka ameneyi…sheeee unapanga political science ndiwe basi
@ dola
Ndizija mumanyoza nazo pope. Focus on issues and not personality. The issue here is not about one being tumbuka or tonga (ngati ine) or LOMWE ngati manganya no. It’s about government and DPP led by mutharika unleashing mchacha to terrorise Malawians.
Koma atumbuka simutopa. Mmene mudayambira muja? Tiye nazoni poti that’s where you belong, kumayenda mmiseu pamene anzanu akulamula. I am yet to research and find out the meaning of this word mtumbuka.
Dola, zosankhana mitundu ayi please. Sungamve chisoni kuti tatha 54 years, Mulungu kumatipatsa mvula koma palibe chikuchitika. Ineyo ndi mu Lohmwe koma sindikhulupilira zosankhana mitundu.
Kodi mukamati mtumbuka mtumbuka, inu ntundu wanji? Uchitsiru umenewo.
eya ndiwa nzeru…………………………………