Email a copy of 'PP says Joyce Banda has well-founded fear of persecution if she returns to Malawi' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'PP says Joyce Banda has well-founded fear of persecution if she returns to Malawi' to a friend
The High Court in Blantyre has demanded evidence of former president Bakili Muluzi’s Commonwealth involvement after his attorney informed the...
Mutharika did not run away from her persecution, when she arrested him alongside the midnight six. let her come home and have a taste of her own medicine!
I am happy that she is living outside the country because our money is not used to pay her and her security detail and government must forfeit her benefits. Mwana wake ndi yemwe anangomuninkha ntchito ndi uyo yamuthera ku Millenuim Challenge Acccount (MCA). Analira mwana ameneyu ku MASAF kuli Kakhobwe kulephera kuchita develop communication strategy ndiye ati ndi Chief Executive ku MCA, za nkutu.Management yake anakaiphunzirira kuti – munthu wopanda management experience from nowhere angakhale Chief Executive Officer? Kachibwenzinso ka ku Standard Bank ka ku Kenya ndi kaja kanathamangitsidwa kupita ku Zambia chifukwa cha matama.Ntchito amangopasa anzake a kumpoto, shupiti.
Anabadi nanga sakubwera bwanji if she is innocent. The relations kumpukwezi changes lifestyles in midair mpaka kutumiza mwana ku china and yet we were same level.
osangovomela bwanji
It is high time these unpalatable stories circulation stopped. In all fairness, if the allegations are what they are why can’t she come back home? In case the government goes ahead to incarcerate her, there are many lawyers needing clients and many courts to hear her case. The article mentions a number of previous politicians and surprisingly all those mentioned are still residing in Malawi in their own homes; has any of those been sent to prison, why then should it only happen to her? Mr.Msonda is mentioning about Mr. Banda writing letters to the international community complaining and defending… Read more »
Those who live by the sword will die by the sword. Mai mukuthawanji popeza munali ndi mphamvu zoposa mkango nthawi ija? Do you remember Joyce that at one time you said a certain elderly man prophesied that you would do great things in life? Inu muinati mkuluyo adati ‘mweana uyu adzachita zazikulu” Zazikulu zake zinali kuba ndalama ndikuthawira kunja? Dziwani kuti mulandi siuola. Nzani uja ndi uja walamulidwa life imprisonment for commiting crimes gainst humanity ku Senegal. Inunso mukulowera komweko.