Email a copy of 'Prophet Mbewe ‘prophesy’ Vice President convoy accident' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Prophet Mbewe ‘prophesy’ Vice President convoy accident' to a friend
The million-dollar question is whether or not Malawians will ever have a bright future-a future where parents are able to...
F0r God’s sake,these people are not Prophets, they are thieves and lions in sheeps’ skins.If this guy was a Prophet,how could he fail to foretell the predicament that awaiting the VP? In Malawi whom should we trust? The President himself is a thief,his Ministers are thieves and the MPs are a bunch of idiots.OH! LORD,DELIVER US FROM THESE SATANS!!!!!
Baba Chilima musatekeseke ndi anenere onyenga ngati Mbeweyu, Akapanda kunama adya chani pa town. Kunamako ndipo podyera pake.
So how will one pray for a country which he/she doesn’t know? Praying in vacuum? Isaiah, Jeremiah, Samuel etc, the bible prophets we know never beat about the bush when revealing a prophecy to people. I am baffled why today’s prophets are so afraid to tell us specifics of their so called prophecies. Are they even not sure of their own prophecies? Are they afraid of being found out?
MA pali Mauritius Mali Mauritania etc. Prophecy iyi is targetted at our own innocent VP. Zazii basi.
Mukati simuna ntchule zina inu muli dziko lanji? Ndipo chakupasani inu chimdi ndichanu kuti maganizo anu asanduke ulosi powuza dziko. Inu tazingowabela anthu amulungu koma zenje lanu lili pamovuto ndipo sinu neneri. Palibe neneri yemwe analosela kubadwa kwanu. Uthenga oti inu mwabadwa aunabwera ndi gogo wina zina lake Sanudi kukawawuza Malo anu kumusa kwa msewa. Chonde chesani.
Kod ngati inu muli neneli ndi buku lanji likamba zakubwera kwanu! Ndipo ndichizindikilo chanji chomwe mulinacho? Poti nanga ndibuku lanji mwaza nalo lokamba za inu kuti ndi neneli Oh Mbewe upezeni mtima Buku loyera mumapezeka pa Mateyo 24:4 pepani simuzaziwa za mawa. Ndipo inu Mumwalira or patalike bwanji ndipo mukaweluzidwa pomulosela nzanu zonyasa. Kodi ndinu opambana kuposa Angelo? Mafupa anu 360 pomwe Ngelo sawelengeka. Nundi kapolo wa Mulungu Allah dekhani ndipo zinena zowopa mulengi Allah
Ndichifukwa chani simalota zoti baja lawujeni lizasangalala polibe yemwe amaziwa za mawa ndimulungu Allah ekha. Mateyo 24:4 onyenga awa ife timufunila zabwino vp. Ndipo atetezedwa.
Kodi za mkazi uja anapasidwa mimba ndi mneneri David Mbewe zili pati?????
bwanji osalosa za bvula mkumangolosa zabofza .kodi anamuuza kuti nfi Mbusa ndani
Mudziona simunati