Email a copy of 'Protests over ‘death of healthcare system’ held in Rumphi' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

35 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
AGAMA FULOWENZA
8 years ago

Amalawi tili ndi vuto loyiwala msanga. kumbukani kuti ndalama zinabedwa za nkhaninkhani m’boma nthawi ya JB, ndalama zomwe zikanathandiza dziko lathu lino. Pano boma likuvutika kuti lipeze ndalama zoyendetsera ntchito zake. zonsezi mwaiwala kale? kusowa chithandizo cha boma ndi nkhani ya tonse ngati amalawi.sinthawi yolozana dzala.

wayunda
8 years ago

I’m not in support of you.This is country wide agaist Peter. There is no smoke without fire.

kent
kent
8 years ago

MA FELLOW NORTHERNERS WE SHOULD NOT BLAME GOVT.TAKE EXAMPLE OF RALPH KASAMBARA WHAT DID HE DO DURING JBS ERA HE STOLE MONEY THROUGH CASGATE HOW MANY NORTHERNERS WERE INVOLVED IN THAT MASS LOOTING OF GOVT COFFERS.JUST VOTE 4 ME I WILL KILL ALL THE NORHERNERS AND BURN THEIR BELONGINGS IN THE COUNTRY.

Nyapapi
Nyapapi
8 years ago

Why is it that many CSOs and their leaders are Northerners? To say the fact these gurus have an in-built element of evil minds agaist others gvt. To hell with ur protests. You think we in LL will emulate that. Mwagwa nayo basi,

Mbuli
Mbuli
8 years ago

Kuba too much,,,, ine ndili ku Rumphi komkuno koma Sinddayende nawo chifukwa Kuba ndalama Zaboma ndi mabungwe kwakula, komanso kuwonjezera pamene mabungwe ambiri sakuziwa chochita, monga Ophunzitsa achinyata zinthu zosiyanisiyana M’malomwake ogwira ntchito angozilemeletsa Okha- zotsatira zake chomwe achinyamat akuziwa ndikumwa mowa ndikumakavina ku ma Birthiday paty omwe amakhla akuchitika week end iliyose m’malo osachepera 10 patsiku… Chonchi malawi ndikukhala ndimaganizo ofuna kutukuka,,,, ndizomvetsa chisoni kuti Chilichonse anthu akungoti Pulezideti ndimvula yomwe,,, Tiyeni tizikumbukira kuti azipembezo zosiya-siyana timkapemphera kuti Mulungu atipatse Nsogoleli ndiye tiyeni tikawerenge Baibulo ku mayeyu 7:7 kumatsika,, Tiyeni tikhale ndi mtima wa umunthu. Komanso tikonde Dziko lathu…….

masa masina
masa masina
8 years ago

These are the days of survival of the fittest. Days of free lunches are over. There are plenty of drugs in private hospitals.

Mlauzi
Mlauzi
8 years ago

Aganizireni anthu osauka. Empathize with them. Muganizire muli inu. These people cannot afford to pay bills at Mwayiwathu, Seventh Day Adventist or even kupita ku South Africa kapena ku India mumapita inu kuja mukadwala. Misonkho yathu ija mumadula pa salary ndi zinthu zogula ndi ku Road Traffic, ku Immigration ndi zina zimapita kuti. Someday you will pay for the suffering you are causing

Mwendanato
Mwendanato
8 years ago

MBANGE NDA NJUNGA NDA NGOMA ZILA JB WAKAMUGABIALANI NYENGO YA KAMPENI. FUMBANI KAMLEPO WAMUVWIRANI IMWE BINA RUMPHI

Mwalusya kuvotera wamama winu....kkkk
Mwalusya kuvotera wamama winu....kkkk
8 years ago

Sono kuvina uku si mwakhuta kale apa…vindere nadi ivi….

Khima
Khima
8 years ago

Bwanji osayamba kaye mwasonkhesa ufa ndikukapeleka ku chipatala kenako nkukayenda kunseu kusonyeza kuti inu nanu mbali yanu mwachita, isale ya boma??? Tikaonesesa mwinanso nonsenu apa ndi msonkho omwe simudula kupatula VAT nde muli pa fore front…Its time to be logical..tiyeni tidzuke

truth
truth
8 years ago
Reply to  Khima

typical quota reasoning by Khima @24.. You want these people to dig into their pockets to cover peter’s wastage and theft of our own taxes. these people are protesting against theft by DPP and you know that

Read previous post:
Journalist Mzati challenges Mzuni arts students to be creative

Veteran journalist and social commentator Mzati Mkolokosa has challenged students pursuing degrees in various arts disciplines at Mzuzu University (Mzuni)...

Close