Email a copy of 'Radio Maria needs K70 million to extend its transmission in Malawi' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

12 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Khumakhuma
9 years ago

If all the three Million Catholics were to contribute Mk 1,000.00 each this project would not be a problem at all; ngakhale Mk 500, ndi ndalama zambiri to put up this project and sustain the running of the radio for quite a reasonable time. We do allot of contributions in our Parishes, this could be done!

wisdom
wisdom
9 years ago

Kindly consider Muloza-Limbuli in Mulanje

MELINDA
MELINDA
9 years ago

Tisonkha za mpingo wathu izi.

chimwemwe chimtengo
chimwemwe chimtengo
9 years ago

Zimenezo ndiye zofunikazo radioyi ifalikire ponseponse .May God bless u Fr Joseph Kim Amen.

SIMON
SIMON
9 years ago

Zabwino zonse , Fr Kimu you make me proud and i really admire your hard working spirit. Please never be discouraged in all that you are doing for the Church and the country. May the Good Lord, the Almighty bless you abundantly.

Proff. Centvinnie
Proff. Centvinnie
9 years ago

Makamaka muganizire ku Chizumulu ndi Likoma Islands. Ndi kumene kungatalikirane ndi ma transmiterwo. Feasibility study please!!!!

Khongoni Boy
9 years ago

Komaso Kwathu Kuno Kwa Khongoni

Leston P
Leston P
9 years ago

The story of Radio Maria is such a beautiful story. It is the flagship radio in terms of religious radios in Malawi (not just Catholic radios)……. all because of the hard work of Dr Kimu and his team. BUT, do we need 4 catholic radio stations in Malawi (in Mangochi, Lilongwe, Mzuzu and Karonga)? Do we call that a United Catholic Church? We read that in RSA, the Catholic Church which has over 50 dioceses has only 1 radio station – what’s wrong with us? If it is a question of languages, I am sure Radio Maria can accommodate all… Read more »

ANgoni Ngayongayo
ANgoni Ngayongayo
9 years ago

Pitilizani ntchito yabwino yoweta nkhosa za Ambuye ndipo Ambuye Yesu yemweyo azikudalitsani. Ma ulaliki ndi maphunzitso anu amatitsitsimutsa. Timakunyadilani koma chonde kunonso ku Mchinji mutiganizire chifuwa timamvera wailesiyi movutikira kwambiri. Mulungu apitize kukudalitsani ndipo mupitilize kutipemphelera zikomo.

Amuna
Amuna
9 years ago

Ngati n’kotheka muganizirekonso kuno ku kasungu pa boma. wailesiyi simveka bwino.chonde bwerani mudzafufuze.

Read previous post:
Why are white people expats when the rest of us are immigrants?

Surely any person going to work outside their country is an expatriate? But no, the word exclusively applies to white...

Close