Email a copy of 'Robert Chiwamba set to launch new poetry album' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

22 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
M'bujo
M'bujo
8 years ago

Tiyeni tinene ZOONA Abale….kodi to RECITE ndi kutani?

Thomas Mussa
Thomas Mussa
8 years ago

Tonse tikudziwa kuti chilungamo chimawawa koma Dokotala Mtabeni walankhula zoona,it was the same with our musicians (especially gospel musicians) they used to play their CDS in the name of live performance. Malawians quickly realised this raw deal and start asking for live performance. Now things have changed for better.

Geofry mvula
Geofry mvula
8 years ago

U r vry great! keep de brain folding!

Mayamiko Matapa
8 years ago

Adokotala Mutuwanusugwila And Zoti Ndiwe M’malawi Ndakayika Mbuzi Yamunthu Moti Pamenepo Ndipolakwika
Chiwamba Kip It Up.Awoatayeni Adzafa Ifayowawa

bondo
bondo
8 years ago

Malawians let us appreciate others when they do well mmmmh kunyodola basi zaziiiiiiiiiiii……Chiwamba, my favourite

Paul Liphuka
8 years ago

Chiwamba ndi makina a mphepo, amakwanira.

Dokotala Mtabeni
Dokotala Mtabeni
8 years ago

Hear this Mapwiya.Mlakatuli means someone who recite poems from the heart, when one is reading from a copy like what your Robert Chiwamba is doing they cease to be called Mlakatuli.Kupita ndi kupita Ku launch basi kumakaonera munthu akuwerenga mkope?Anyway paja aMalawi we always settle for less.

mapwiya
mapwiya
8 years ago

a dokotala mtabeni, chabwino, inuyo yambani kupanga ‘recite’ ma poem anu from your head tione ngati mungafike pa Chiwamba… Tione ngati athu angabwele ku launch yanu..inxaaa…. Go Chiwamba go!! machine iweyo!! you representing.. ife tili komko to support you chibey!

levelheaded
8 years ago

Umatha composition koma the way you recite zazii. Too much kachibwanabwana mwina poti umayelekeza udakali Ku college. Ine favourite wanga ndi uja amati kunkhondo tea amamwera mjombo kutakasira nfuti. The way he recites ndi chichewa he uses, very talentful. Okoma àtani kuchulukitsa zolira.

Tman
Tman
8 years ago

Great man of the moment. Keep the fire ???? burning

Read previous post:
Three girls sexually assaulted, impregnated in Lilongwe: 3 arrested

A businessman, a primary school teacher and an old man are currently in police custody in Lilongwe for allegedly defiling...

Close