Email a copy of 'SADC forms new Tribunal, Lake Malawi border row quashed' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'SADC forms new Tribunal, Lake Malawi border row quashed' to a friend
Ministry of Gender, Child, Disability and Social welfare Patricia Kaliati has advised people in Karonga to maintain their Members of...
When peace fails,use defence…
as malawians being patient on the lake issue doest mean we r cowards. all avenues have not yet been exhausted .more fire Dr Chaponda.
Sindine sapota wa DPP, koma Dr Chaponda kumeneko ndiye kuyankha,komanso iwe nambala 7 Dadaboma sindiwe wa kumpoto ndiponso sindiwe M’malawi,ine ndine wa kumpoto ndiponso ndikudziwa wa kumpoto sanganene nchoncho,ineyo nditabvutika kwina kwake kaya ku maiko akunja mu lhomwe kapena wakumwera akhoza kundithandiza kuposa wa ku Tz.
Dadaboma is not a Malawian. You must not confuse us malawians on this issue and let alone the northerners. This is not a Lomwe issue. Dadaboma, youi are uncouthed.
Dr Chaponda, the man behind the Farting Bill to ban people from Farting in public. A”Dr”, amunamuna amenewo.
Chaponda is contradicting the already established facts. Malawi is a complainant because she feels TZ is laying a false claim to the northern half of Lake Nyasa. Therefore Malawi is complaining as she thinks TZ wants to usurp its property. Because of this Malawi went to seek the arbitration of courts or other interim bodies. Malawi is an obvious complainant in this. Why is Chaponda saying the opposite, and why are his stupid Lomwes clapping hands for him? Let me say categorically that half of this Lake truly belongs to TZ and we northern Malawians are in full support of… Read more »
Kumeneko nde kuyankha kwachimuna osati zonyengelerazo. Mai kumene muliko mukumva bwa? Mwinatu munkafuna kt muiphetse za cashgate zitayamba kukucheperani. Shame!!!
Uku nde kulakhula kwa amuna osati aja amafuna kutibetsera nyanja aja
Dr.George Chaponda, B.A(History), LL.B(hons), MA(history), LL.M, Ph.D
He said kuti wecan win without the northern region
Boma la amunamuna limenelo,munthu opita ku khoti ndiyemwe zamudinya osati eniakefe.
kodi munthu akasilira mkazi wako ndiye kuti ukasume? kapena maiwa anali ndi cholinga.