Email a copy of 'Simbi to build Malawi's tallest ‘twin towers’ in Lilongwe' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Simbi to build Malawi's tallest ‘twin towers’ in Lilongwe' to a friend
TNM through its mobile money service, Mpamba has come to the rescue of Thambe Primary School by building a teachers’...
This is what we call true patriotism to one’s country. Osati kubwera kunja nkumakaba ndalama za a Malawi osauka nkumatukwana kuti mudabwera olemera yet there is nothing to show that you were there. Your accounts only to become fat while in a poor government. Shame on you shameless, hardheartened thieves. Mulungu adzachita nanu.
major one please consider investing in Malawi along presidential highway city centre
Why are people and organizations challenging Zitukuko zabwino ngati izi? Vuto lanu ndi chanu kumupanga support munthu kuti chitukuko chitheke? koma dzikoli lidzatukuka ndi dyera lake limenero?
These are good developments which we can all not stop smiling at.
But are issues of fire safety being taken into account? If an inferno was to break out on those to floors would our fire service be able to contain the situation?
Is our fire brigade being modernised in tune with these high rise buildings?
Akanakhala kuti chitukuko chimenechi wanena ndi Peter Mutharika bwezi zitsiru zina zikuti ndi campaign. Simwangokhala phwii kumeneko ngati mukumetedwa? chitantu comment anapa***o inu.
hahahahahaha koma …izi za cooperate world osati zandale zakozo! ah
Chitani manyazi wawa….you seem to be a diehard supporter of DPP and that wont help.
Apa Pitala zamukhudzanso pati? Komatu u Kadeti ukukuzunzani..
Kikkkkk koma Dzombe iliso???????????????????? uzichita manyazi wanva? kupeza mwayi wopanga comment pano sitikuti tilipano kuti tigule uchisiru wanuyo mwanva? Khalidwe lachikalekale basi?
why can they not do the same in mzuzu and zomba since we already have decent buildings in lilongwe and blantyre
Iweyo umange ku Zomba ndi Mzuzu. Simbi akumanaga ku Lilongwe -Capital city of Malawi
Wow that can change the face of the capital and we may start calling it Capital city and the structure can have a ripple effect to ignite other investors to build even better and taller infrastucture in our Capital city. Amalawi tiyeni timpaseko mpata Simbiyu mwina ndalama zake zitha kutukula miyoyo ya a Malawi ambiri.