Email a copy of 'Sithole found guilty of cashgate; sentencing adjourned to Oct 28' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Sithole found guilty of cashgate; sentencing adjourned to Oct 28' to a friend
The High Court in Zomba has dismissed former President Joyce Banda's injunction stopping main cashgate suspect Osward Lutepo accessing her...
Akhale dzaka 100 kut tikokere kumene anadyako mbava zazkulu ngat zmenez,agalu!
koma a polisi olembedwa ndi a mathanyula, manja m’thumba choncho koma akuperekeza mbava yayikulu ngati imeneyi. pa nyasaland amwene!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!!
PP Thugs, can they expose the big fish too apa!! it is about time, she is busy jumping to other countries she better come and face the law!!
pi piiii !!!! odi uko amayi aduseko ndi wa chiwili wawo(zingayambe kuyiwalika) munya simunati
wa Policeyo analembedwa ndi Peter.. mwaiwala kuti nthawi ya campagn ankangowatenga ndikuwalowesa ku PTS ku kanjedza
Koma waPoliceyo zoona kupisira manja m’thumba choncho?…Akuti SWAGGA mwini wakeyo…Zili pa Nyasaland
At 26 and a house in area 47. Mwana anatasa ndi misonkho yathu uyu. Watsala Namata and Nantchito both mansion owners while most of us are strugglers. Area 6 where Maula Prison is located is waiting for you. Leonard Kalonga will have no chance for women and the title of Nyapala is waiting for you there together with Joster Njanji.
mpandeni wakubayo asala auntgate munya utsi mumadeweza kkkkkkkk
10 years imprisonment with kalavula Deya would be befitting sentence for this youthful thief
Malamulo a pa malawi ndi 0 pa hundred how come Lawyer Kasambara akuyimbidwa the same mulandu ali ndi ufuru oyimila anzake mulandu ofanana this is rabish these are thieves and Muhura is busy deffending mbava zoonekeratu ali mbava nayeso rotten country you need a wise to catch thieves osati tulo mulinato mu dziko muno changamukani a malawi.