Email a copy of 'South African king reveals xenophobia plan: Malawi immigrants beware!' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'South African king reveals xenophobia plan: Malawi immigrants beware!' to a friend
Malawi's parliament is expected to reconvene next week Tuesday for a budget session, its Speaker Richard Msowoya has said. The...
Kwa eni kulibe nkuwo kumadyesa nthanga dzungu ukulifuna, kabwelaniko kwanu ndikuno nawo azaziwona
My fellow malawians in RSA jst come back home.kwa eni kulibe mkuwo,osakakamira kwa eni ngati kuno munaphako munthu-bwerani tidzathandizane kulima
I t’ink Zwelithini iz a zombie of some kind !
His speeches & coments ‘re counterprodutive!
Zwelithini is not human even Thabo Mbeki was educated at Chanco in Zomba.
Amalawi kudzikonda, chifukwa choti muli ndi mwayi opeza tindalama ku Malawi konko ndiye muli bizzy ku komenta Za nyansi kuona ngati tonse tidzipanga zimodzi,
Pelekani maganizo anzeru tikuombereni mmanja osati zonyoza .
I salute the king for being innovative.Its unfair to live hardlife in own country due to rapid population growth caused by foreigners who do not have permision to live in country.Malawian leaders should learn from this.Illegal migrants r supposed to be entertained they bring negative change.MABULUNDI AKUCHITA CHIPONGWE OPANDA NDI MAKALATA OMWE OKHALIRA DZIKO MUNO IFE MASO TONG’O.
AMW KHALANI MUDZIKO MWANU CHONDE
We shall see how it works
God help us. Amen
Mau amzeru achawa mudaonjeza kumangopita kumangodzitsa ang’anga akwanu basi?