Email a copy of 'State House sidelines Viola as Mutharika launches Lilongwe by-pass road' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'State House sidelines Viola as Mutharika launches Lilongwe by-pass road' to a friend
There is nothing wrong with cigarette manufacturing firm—Nyasa Manufacturing Company (NMC) – to be bankrolling Malawi champions Big Bullets FC,...
Develop Lilongwe but ochewa kaya zanu inzoooooo come 2019
Is it Mr Viola who would be always master of ceremonies in each and every meetings that the State President will be hosting? why you did not say anything about the Salima rally whereby Mr Mwamsambo was a master of ceremonies? Its a total lie to say that most truch drivers are shunning the road, I myself have witnessed a lot of trucks using the road even as far as from kanengo area. Should we say that the President is not in good terms with his personal assistant on religious affairs if the prayers is given to someone else apart… Read more »
Malawi siitukuka ayi. Zoona president mpaka kusegula musewu wa 13 kilometers yokha. Anzanu misewu ngati yotere amatsegulira ndi nduna. Shame
anyasa ngati sim’mafuna kulemba zachitukuko, maka by DPP, bwanji osamangosiya.. msewu ndiwandalama zingati, colon pa ndalama akupangapochani? mukufuna kuchepsa chitukuko eti? msewu mungamange ndi ndalama zochepa mwalembazo! kkk koma chidzaphulika tsiku lina dithu, eee! anyasa nanu musanduka chipani ngati ma cso kkk koma greedy at its best
This country where chiefs are busy declaring they belong to the ruling party is patheic. Chiefs have not yet understood that by virtue they are already far above party politics. Chiefs find themselves worshipping political leaders….eeish. As a chief you can simply say your words of thanking government for the road constructed, you then ask other government ministries for water, etc. And the. You ask your subordinated and the general populace to take car of the road infrastructure. You tell your people to stop attacking vehicles using the road as has been case over the past year. You ask people… Read more »
No 10 uli ndi miyendo ingati?ndiwe openga kwabasibasi lol lol
A mfumu a Malili asatengeke msanga iri ndi dziko lozungulira. Mafumu sayenera kukhala ndi mbali chifukwa amapanikiza anthu. Nanga ntchito za boma agwire ntchito ndi a boma koma pakafika nthawi ya chipani sayenera kuonetsera kuti alu mbali iti. Nsewo wo by pass ndi project ya kalekale. Ine ndinayamba kuimva mzaka za mma 80s. Komanso mseu uwu anaika mwala wa maziko anali a PP. Tiyeni tizichita chilungamo. Mabvuto ena tikukumana nawowa ndi chifukwa chopanda chitsogozo cha Mulungu. Tiyeni tichite ngati anzathu a ku Zambia omwe chuma chawo chiliko bwino kusiyana ndi ife koma anatseka ma bala tsiku lathunthu kuti apemphere. Mulungu… Read more »
Uyu ndiye President wangawanga!;!
Kodi amalawife tizidya misewuyo. Nkhani ya njala ukuti nayo bwanji.
Zakumachende basi!!!! Malata ndi cement zotsika mtengo zija zili kuti?