Email a copy of 'Supreme Court of Malawi set to give verdict on DPP, Karim case Sept 14' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Supreme Court of Malawi set to give verdict on DPP, Karim case Sept 14' to a friend
Pollster, the Malawi Electoral Commission (MEC) has ruled out the population and census which has started on Monday across the...
We have a president who is a thief and is not ashamed of stealing at the age of 80. His wife is a crook too and is possibility forcing the old man into theft. She is building flats at Ntaya near Bunda Turn off and a road is being constructed to the flats using tax payers money. Do CSO know this? Do opposition parties know this kapena mungodziwa Kudya chips cha pa chiwaya nkuwonetsa luso logenda legeni nkumanama kuti mudzalemba anthu one million? Ugalu bwanu a utm.
Koma nsanje yakoyo uphulika nayo. Tapita mmizindamu uone nyumba zomwe enafe tikumanga using our own sweat. Inu mukulimbana ndi amene zawo zidayera kale. Siyani nsanje pangani zanu. Ya njiru siswa madzira. Next year another cry of atibera in the pipeline. Choona ndi chomwe wanenacho. Anthu asaduduluke ndi moto wa mapesi anthu mizimu akudziwa kuti saapala. Disgruntled Kaliati, Callista and Chilima will be shamed to extremes come next year.