Email a copy of 'Tempers flare at PAC conference over regime change calls: Wandale wants 'corrupt' Malawi govt suspended, Ntaba says DPP can't leave power 'we can be worse'' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

25 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Jamax
Jamax
6 years ago

Kodi foreigner uyu akuti chaniiii???? ma pulezidenti anzake apita kunja kwa Azungu kukalankhula mfundo zachitukuko bwanji nanga simunapite??? kkkkkk!!!!!…..by the way makobidi omwe munatenga kwa anthu aja mabweza????? kkkk!!! Wa Ndaleeeeeeeee!!

nophiya
nophiya
6 years ago

Go PAC. Go Pac. More fire

Gonapamuhanya
Gonapamuhanya
6 years ago

Why people are not talking about corruption in the civil society, in churches, private institutions and the church/mosque? Do you know that most of those who are making noise have amassed wealth corruptly? If we follow up church leaders, you will see that they have assets that were obtained corruptly. Some have empires with assets distributed amongst relatives. How I wish we had investigative journalists who could track religious leaders. We could be stunned to know that they have things that they acquired corruptly and some of them have children with women with whom they cohabited corruptly. Easy to point… Read more »

wakikikiki
6 years ago

Tiyeni amalawi tichangamuke , tidzuke mu tulo , Wandale siwopusa, wopusa ndi amene asutsana naye . Chifukwa chofuna cha Wandale sakuchivesa. Akufunika civic education kuti mwina zingalowe mmutu. Minda azungu anatenga liti? ndipo nthawi imeneyo anthu analipo angati? panopa tilipo angati? Nde musove samuyo mupeza kuti zativuta kale . Chofunika nkutenga minda yathuyo tizilima eni ake . Awandale ndili pa mbuyo panu tiyeni nazoni. Ngati mtsogoleri akulephela kutenga mindayo monga mmene anapangila Mgabe ku Zimbabwe nde utsogoleri uli pati?

nyopex
6 years ago

APM ali pheeeeee kunyumba yachifumu ku Lilongwe. And all of us know kuti zake (APM) zinayera kale. Enanu baavutikani ndi mtimawo ife 2019 tidzavoterabe APM.

Ndiye APM akadzawinanso 2019 muzizati wabera agalu inu and yet you see how well he is governing this country. Mulira simunati.

As for Wandale and Maya, and Kamulepo, these are the three mad people that are not yet gone to Zomba Mental Hospital due to too much smoking of weed(chamba)

wakikikiki
6 years ago

Antaba anawakana kale kwawo komwe. Anayesela kuyima pa u MP anthu anati ayi simunthu . Nde lelo anganene chani cha nzeru. Adaphadi Bingu ameneyu, sankamuwuza zoona prezidenti wanga wokondedwa.

MALITINO FROM BAGDAD LL
MALITINO FROM BAGDAD LL
6 years ago

ENANU MUKALAMBA OPANDA FUNDO, KODI A PAC ANATIYANITSA MSONKHANOWU FOR THAT ISSUE.NEXT TIME TRY KUKAMBIRANA ,AIN ISSUES ONLY,ONLY ONE KING RULES AT ATIME PAITIENT;Y WAIT FOR FOR YOURS IF AT ALL WILL HAPPEN.

Lazalo
Lazalo
6 years ago

Non PAC members are not supposed to make any contribution at the meeting, I quote ArchiBishop Thomas Msusa. So Wandale and Mayaya’s contributions are void. Read the last four paragraphs carefully and unbiasely.

mo
mo
6 years ago

First suspend NRB its a tool for Dpp to steal ur votes,open up oposition open up Pac,they will use the same came 2019 mind we have census in 2018 another stone,azawina mwa mai wawayeeee listen carefully to Dausi if u cant c pls open ur eyes

mlomwe
mlomwe
6 years ago

Following keenly

Read previous post:
Malawi Chief Elections Officer dies after collapsing at work

Malawi Electoral Commission (Mec) acting Chief Elections Officer, Thandie Mkovole has died after she collapsed at work this afternoon, it...

Close