Email a copy of 'Ten Malawi police officers arrested for stealing' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Ten Malawi police officers arrested for stealing' to a friend
The Chewa Heritage Foundation (CHEFO), a cultural and charitable grouping has responded to support calls to hailstorms and floods victims...
Low pay is no an issue be oz when applying for the job we are told the conditions and terms.ngati sumuyifuna umasiya
Ine ndiye sindimadalira za ma POLISI zanuzo, polisiwanga ndi YESU ,ndi agero ake basi, osati omanunkha khwema poyendawa,
Wow. I can’t believe this. How could law enforcers break the law.We can not blame much may be they earn peanuts. Government step up and solve the crisis. Punish them to make lesson for other law brokers
I’m sorry guyz ,use athief to cache a thief
Khondo nd anas nd anthu amwewa amene amabweka akuba mfut kut kumatbera manyumbam
unfair&unacceptable behaviour,law enforcers why?
Wa Police wina aliyense ndi wakuba,waziphuphu komanso wakupha dziko lonse lapansi.Kusagwidwa kokha ndi kumene kumawabisa maka kuti tsiku lawo limakhala lisanakwane
umphawi wathu amalawi pano nde wawonekela patali apolice abe,akuluakulu amboma abe, ampingo abe ngakhale mtsogoleli wa dziko amene abe nde athetse umphawi wathu ndindani? ngati dziko latilephela tingoligulitsa ku nearby country
SO WHO IS GOING TO PROTECT THE PUBLIC, SORRY POLICE
A police akumaba kwambiri ponamizira kugwira anthu omwa ma sachet, e.g a police apawenela ku blanyre, akagwira munthu bcoz of sachet akumusiya akawapasa k 2000