Email a copy of 'The Malawi ‘WhatsApp coup plot’' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

43 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
enock Sakala0
enock Sakala0
8 years ago

Whau our land has turn into a battle fied God come now to take me before it becomes worse.politicians are chamerions’thieves, and liars why my mother having problems cos of our stupid leadership

tondewakufa
tondewakufa
8 years ago

yayi odala msatero okumanga,wanthuwatu soluchedza ukwidzinga

Luke
8 years ago

lne ndiye ndiyankhula basi a MACRA nambala yanga ndi imeneyi mumpatse Dausi akapeleke kwa bwana wake. posachedwapa ndinapita ku chipatala koma zachisoni anthu kumabwerera panado wachabechabeyu kusowa, odwala kumauzidwa kuti agule? ndalama azitenga kuti? ndiye inu a Dpp muli busy kumanga anthu chifukwa cha kuyankhula chilungamu?, dyera mtuni koma pasafike pa 2019. NOTE: ndakamba za Dpp osati boma mukafuna mulandu ndikakuyankha iweyo Dausi.

chochi
chochi
8 years ago

Welcome jelbin mk we missed you. Of course it is the two judges who actually sent Kabwila and friends to discuss regime change on whats app. They also caused hunger in Malawi. And they made your party to lose in the southern region. Shame !

anonymous2114
anonymous2114
8 years ago

Freedom fighters? Are u crius…. They are getting bail nw wat if u do the demos are get arrested they will bail each other and leave u there. Am not a politics guy but ril guys all this is jxt politics it has nothing to do with other ppo suffering as long as they hav the power they are fine… Let’s stop listening to these politicians and build our own malawi , if this continues one day there shall b war n those suffering shall b us not them

Chatsika
8 years ago

Ahh! I don’t see any case here as former director of public prosecution. Treason? My foot. To hell with your charges. Ndiye bola akanamanga Gwanda chakuamba uja ankati alowa mtchire uja. CIRMS ija ankakana kuti akufuna kuti adziona zokambirana zaanthu ija ndimeneyo. Ndiye mutimanga ambiri. Koma mwati awa sadzimva zimene tukambirana kubedi. Koma Dausi eeee

patrick joseph sizala
patrick joseph sizala
8 years ago

i dont c any case/issue lets wait 4 de court 2 judge

brie
brie
8 years ago

aaaaa ine nde sundikuona chomwe awamangira….

aaaa seriously? presidential advisors gv proper advice to ur bosss pliz,…..

mzungumbuli
mzungumbuli
8 years ago

Lets shun away from using Airtel numbers. Airtel ili ngati Yudasi iskariot idzakuperekani lets go for TNM guys.

JUSTICE KAMWANA
JUSTICE KAMWANA
8 years ago

kODI PULANI MUKUPANGAYO NDI YA AMALAWI KAPENE MABANJA ANU. ZOMWE MUKUIKA PATSOGOLO NDI PHINDU LANU BASI. ANYAMATA MUKUWAFUNA KUTI MACHITE NAWO ZIWAWAWO AKAZAGENDA APOLISI PENA APOLISI NDIKUTOPA NDIKUWAOMBERA MUKUTANTHAUZA KUTI MUZABWEZELETSA MOYO WAO ANTHU OYIPA INU MUZIOPA MULUNGU NDALE ZAMTUNDU WANJI ZIMENEZO KOMA MUMAPEZAKO NTHAWI NDIKUMAPEMPHERA AKABWIRA NDI ANZANU GOD FORBIDE CHAKWERA AND YOUR PATY GOD CAN NOT ALLOW YOU TO BE LEADER OF MALAWI. TSONO MUKUONA NGATI PETERYO AKHONZA KUNGOKHALA PHEEE KUMATI MWAPANGA TIMAGULU TANU TOLANDA DZIKO ZOONA MAPETO AKE MUKAYAMBA KUBWEZELANA CHIKHALA CHANI SINKHONDO IMENENEYO. ZIMENE MUKUKAMBIRANAZO MAFUMU AKUKUZIDZIWA NANGA ENI DZIKO AMALAWI AKUZIDZIWA KUNOTU SI KU EGUPUTO… Read more »

Read previous post:
Uladi storms Malawi Police station in ‘solidarity’: Msungama charged with sedition

A prominent Malawi Congress Party (MCP) official, Ulemu Msungama, has been charged with sedition over a conversation on WhatsApp that...

Close