Email a copy of 'Tobacco farmers expect better price as Malawi sales open' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Tobacco farmers expect better price as Malawi sales open' to a friend
Government has nullified Chitipa’s acting District Commissioner’s (DC) promotion – effected during President Joyce Banda’s regime in 2013 – on...
Muwabereso alimi agalu inu
owo
Akuba anthu agulawo
Commentndikhulupilira Anganyawa chaka chino aperekako madola oyenera, molingana ndi m’mene fodya alili.
Let’s wait and see.
Commentyou buyers be fair enough God is watching you
Its good news to hear. Alimi ayenera asangalale. Boma limafunika chonchi. Zikomo a president Muthalika. Malawi yiri paumphawi wazaoneni. Ana a Malawi ali dziko lonse la pansi chifukwa chothawa umphawi. Pitilizani ntchito za bwino a President Muthalika.
CommentZA MCP ZIDATIKWANA KALE SIMUDZATENGASO BOMA MUIWALE
Musatinamize, tamva kale pa wailesi kuti mitengo ya fodya ikhala pakati pa 85 cents ndi $2.50 amvekere mvula siinagwe bwino.
Kodi chaka ndi chaka mitengo yake nthawi zonse imakhala yoberanayi chifukwa chiyani?
Koma fodyayo akalowa mpaketi, olo kuti mvula siinagwe bwino, ma paketi awo afodyawo sikudula kwake. Peter Stewva… cigarette mpaka K1500 paquet. Zoona?
AZUNGU NDI OKUBA
Osanamizapo anthu apa lowest quality ndi 85cents osati 1.75 amakukochani ndi ndani kodi