Email a copy of 'Two arrested on failed K20m albino son sell' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Two arrested on failed K20m albino son sell' to a friend
President Peter Mutharika presented a moving speech at the United Nations General Assembly in New York which had substance. I...
Hahahaha hustle hard hahaha
I know of one albino who is a nurse… I know of one albino who is a teacher… I know of one albino who is a director of one organisation… I know of one albino who is working at National archives… I hav many learners who are albinos that I support in my profession… If all the parents of these albinos had a kind of a heart like that of a woman from Mzimba, It means Malawi would hav lacked lawyers, nurses, teachers, technicians who are also albinos! Where is this ship called ‘Malawi’ going to? I cry for my… Read more »
Ambuye azaweluza yekha
Umbuli uwu muzonse mmapephelo angakhale kundalama,Kodi million mkupambana moyo wamunthu?Amalawi chikhalidwe chathu chikupita kuti.Akafele kundende amenewo.
Amafuna adye zambiri ndiyeyo mzimayiyo chifukwa chake anakaulura
Chigawo cha kumpoto ndi Tz 2 agalu amenewa amangidwe x4.
No bail to be granted to these foolish people.
Osawamvera chisoni. They are supposed to be given life imprisonment or death sentence.Everyone has the right to life.
A Malawi chikondi chija chapita kuti? Dzoona ndithu kugulitsa mwana kuti akaphedwe chifukwa choti mukufuna ndalama ?ai msatero abale anzanga dziko lino ndi latonse.komanso kumbukirani kuti kumwamba kukuyang’ana inu nonse tsiku likubwera lotentha ngati moto,ndikwabwino m’bale wanga kutembenukira kwa Ambuye wathu Yesu Khristu.
All this is due to poverty. Life is tough in nyasaland yet the president is spending at his will.