Email a copy of 'Two Malawi police officers arrested for robbing Zambian woman' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Two Malawi police officers arrested for robbing Zambian woman' to a friend
M'Methiwa Primary School in the area of Traditional Authority Kapichi in Thyolo district has become the latest beneficiary of TNM’s life-changing Ufulu@50...
FOR YOUR OWN INFO. KU ULIWA MAFUMU ANALAMULA ANTHH AWO KUTI ONCE AGWIRA WAKUBA ACHITE NAYE MUMENE ANGAFUNIRE BUT SHUD NEVER TAKE AKUBAWO KU POLISI CHIFUKWA ENA OMWE ALI NKUBA NDI APOLISI AMENE! I REALLY LIKE THIS ! WHY CANT MALAWI INTERODUCE SHALIAH LAW! OR SHOOT TO KILL!
atuluseni
The possession of game trophie is an offence ,let the Police officers free and again the woman is also involved in corrupting the officers.
Anyöngedwe
Padusanso chinyengo pamenepa,chifukwa chani m’mayiyonso sanamumange?chifukwa apolicewo sanapite kunyumba kwake ndipo ndalamazo anawapasa ngati ziphuphu kuti amusiye,apolice akunchinjiwo mayiyo waangwirisa chinachake.
Ngati ndalama zikuwachepela a police wo osasintha career bwanji? Ndani samadziwa kuti mboma mulibe ndalama? Zonse abazo bwanji osadzilipilila school? Langison ku Limbe police ndi wakuba kowopsya, plis deal with him afufuzidwe. Alwas kwa kachere kubera anthu mdzina la police, timukazinga msiyeni.
Nthawi yonseyi takhala tikuvutika not knowing ndi a police athu omwewa amene akutivulaza. Onse a police pa malawi pano amacheza ndi mbava no wonder samagwidwa akaba akubawo. A man was killed in BCA and the police arrived after 2 hours. The robbers snatched the rifle , a licencd one from the deceased koma mpakana pano siinapezeke. Timve zenizeni
WHY POLICE SPOIL YOUR NAME MONEY NOTYOUR US U DEMAND RESPECT YOUR WORK ROB PEOPLE NOT GOOD NOW U R IN JAIL WHY NOT LOVE YOUR WORK U LOVE MONEY
anthu oipa inu…akawalala ,askaweza …mboli xanu ‘panyini panu…dzulo mwandimenya kwambili..ndepoti ndaxiwa kumene mumakhala nose ndikupexani…aFisi inu…Mapwala anu Nonse Ku Police ko
muxingo chita Ngozi simuma nyela mwano
Choncho
.
Apolice ndi akuba komanso opanda chisoni, mbava akulephera kuzigwira chifukwa amabera limodzi. Ndiye ati pofuna kuwonetsa kuti akugwira ntchito akumapita mma bar amene ayiniake ndi osantchuka ndikumakagwiramo anthu okumwa mowa . Akatelo aziwakolopora dolla ati adzipulumutse. Kodi vakabu yanuyo bwanji simumakagwira ku Chez ku Sterio kapena pa station olo new casabulanca? Mumafuna kuwabera anthu osauka podziwa kuti alibe chilichonse sangakutengereni ku court. Olemera mumawawopa. Vakabu yanji yongogwira anthu oyenda pansi okhaokha koma ammagalimoto ayi? Apolice okuba inu mumangana simunati.