Email a copy of 'Uladi presses for Joyce Banda benefits as Malawi ex-president' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Uladi presses for Joyce Banda benefits as Malawi ex-president' to a friend
Malawi Congress Party (MCP)president Lazarus Chakwera has asked the government to speed up electoral law amendments that should include changing...
As long as she is still abroad, shut up all issues relating to her,especially abt her benefits.
Chikhale chifukwa chosabwelela kuno kwawo chimenecho? Chamba eti,
Kanyimbi no. 22 Do you really know malamulo aku Malawi. Wandidabwitsa kwambiri. A Mayi Banda tikuyenera kuwapatsa zawo ngati dziko. Ndalama zake siza chipani ichi kapena icho therefore pasalowe ndale apa please chonde.
akuyenera kupasidwa ulemu woyenera monga mwa lamuro osatengera mangawa nanunso mukazapuma muzafuna benefits .Malawi woyee!!!!.
It’s true Joyce Banda found Malawi at her lowest point but she managed to bring her up. But this man is failing to do what a woman did in a shortest period. He has no qualities of leadership and donors are not happy with him.
I don’t think most people understand the law very clearly. Our Republican does not make provision for an Acting President. “Where there is a vacancy in the Office of the President, the First Vice President shall take over and finish the term”. Once the Presidential Oath of office has been administered in accordance with our Republican Constitution that person becomes President and is automatically entitled to any benefits that come with the office. As such Her Excellency Dr Joyce Banda served as President of the Republic of Malawi and as such she is entitled to benefits. What if Vice-President Chilima… Read more »
If this is true, this is a blatant contravention of the republican constitution. Regardless of where Banda is, she deserves her benefits. If govt has issues with her, file charges and let the courts bar her from getting her benefits. Its a bad precedent. I fear you may reap what you sow not long down the line.
Petulo mpaseni mayiyu ulemu wake woyenela ngati muthu wopuma nkhale tikuziwa kuti anatibela zambiri komanso ankuzunzani bwana ine monga muthu wa DPP ndikadakonda kuti mumpase ulemu wonse sikuti azawinanso ngakhale apange mwanowakewo please give her all what is due for her. Iwenso Joyce usapange mwano kwa petulo chifukwa padakali pano ndiye mwini munda ukumayenda kunjako kumanena maboza kuti ife tizivutika kodi man Tcheya mayesa amnyozela momuno osati kumauza madonors kuti asatipase ndalama sopano ndalama zimene ukufuna iwe zichokela kuti ndiyankhe kapena upepese kwa tonse amene sitinakupase voti chifukwa 2019 suzapeza mphungu ngakhale zitatani ndanena ndanena ngati ndalakwa ndikhulukileni madam former… Read more »
The girl was an acting state president. So I do not think there is a provision for benefits of retired acting state presidents. Please be conversant with the law. She deserves nothing moreover she has brought more trouble to Malawians.
Meaning the whole JB alibe galimoto olo kungofuna kuononga zaboma monga mwachikhalidwe chake???