Email a copy of 'Vendors clash with police in Malawi capital city: Fire tear gas' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

38 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
clement
clement
9 years ago

Ok, achewa mwayamba kuyerekedwa? Mukuiwara kuti anthu akumwera omwewo ndi amene akuipanga Lilongwe kuti ioneke bwino.Ngati izi muipitiliza tisamutsa likulu kupitanso ku Zomba or Blantyre ndipo nzotheka.Kukumangirani parliament,Stadium,presidetial villa etc mukuona ngati mwafikapo? Mbole zanu mwamva.Mwaila kuti Kamuzu amakakamira kumwera chifukwa chokongola Bt + Kuchawe.Mudzakalira tsiku lina.

ulendowu ndi watonse
ulendowu ndi watonse
9 years ago

tsakulaninso ma besi ajatu kuti enawa akaphuzire maluso osiyanasiyana aja ndi kumapeza chochita . kodi nanga aliyense akakhala venda malo ake achoka kuti , bola kubesiko asakagwirenso mifuti ayi .but the idea was good.anthu koma adangokhala osakhululuka mumaona ngatikuti chilichonse amapanga KAMUZU chinali choipa komatu Ulendowu ndi wa tonse

Agalu Pa Mpando (APM)
Agalu Pa Mpando (APM)
9 years ago

Shaaaa ma venda akwa goliati bwererani mundichitsa manyazi pilizi. Ma venda a ku machinga kapitani kwa kapoloma. Kuno ndi kwa chakwera ndi abale ake a chewa ndi atumbuka

Chatty Man
Chatty Man
9 years ago

Just give them fines if found on street selling items thats all, they will stop all that rubbish!

victim Chamkhuni Lwazazi
victim Chamkhuni Lwazazi
9 years ago

No vendors cannot just occupy places anywhere they like. It’s illegal. But Lilongwe city officials do even worse things. The occupy plots all over for personal buildings or for eventual sale. Investigate the two friends – The Director of Finance (Mr Sibande) – A plot in Area 25, another in new Area 49, another in Area 43, two in Area 47 (one annexing old grave yard near Chigoneka Community Day Sec. school, another one along the same branching road, where he stays, just to mention but a few). The his friend the Chief Executive (Mr Hara) – Oh! plots everywhere… Read more »

Mzika ya Lilongwe
9 years ago

Ambiriwa ndiwobwera kuchokera kumwera kosowa zochita. Kuba ndiye kwawo. Geni ya ma sweet usiku kuba.

gaba
gaba
9 years ago

mbava zachoka kwa goliati
kumadzavutitsana ndi apolice kuno ku lilongwe.fwetseki

zangazokha
zangazokha
9 years ago
Reply to  gaba

Anthu akwagoliati wawo ndi ulimi ndi ma ofice basi, kuima misewu kumabela anthu amaona zotaisa nthawi. Mlesi nchewa kwake nkuvina gule basi akatopa ndi gule nkumabela wanthu ntwn, Nate ntumbuka xul ikamukanika kuthawa Ku kaya nkuzapisa wanthu mmatumba musova!

Chimwamowa
Chimwamowa
9 years ago

Azikuphulitsani Chomcho Mukuzolowela

Mashon chimta
9 years ago

Tinapumulako tear gas

Fathi Alshdhaab
Fathi Alshdhaab
9 years ago

pAja amapita ku chibvomezi or landslide ndi mfuti!
mavendof enawa si an hto ama bwanaku office..kale evdn ma line a mhc panalube zifha.ndala zogulitsa second cloghes or makala or mandazi etc zinali boo zinthu ndi a ngaazi hkb

Read previous post:
TNM pumps K15m for Bullets CAF Comoros trip: ‘Always with you’

Despite Big Bullets rejecting  TNM’s offer to run an SMS promotion to enable the club raise funds for their CAF Champions...

Close