Email a copy of 'Villagers attack train for wheat as hunger continues to bite Malawi' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Villagers attack train for wheat as hunger continues to bite Malawi' to a friend
University of Pretoria striker Atusaye Nyondo is finally fit after a few weeks out with an injury which he sustained...
Jjjjkkk
Amabungwe awuzeni ma vendor azigulitsa chimanga mwa ntendele chimanga tilinacho ma vendor osatiso chanu cha ku Admark kwanuko koma chomwe timasunga pa chaka chili chose
Our Governor Chuka is busy devaluing the kwacha and he should know these are the effects for that, when there is drought you dont depreciate the kwacha to unimaginable levels, you stabilise so people can afford to pay for imported mazie flour. Here this is a double blow malawians drought which is not in our control, but excessive depreciation was in our control, but our governor is against that it seems he wants to punish malawians to the grave.
Hahahaha Boma ilo!!! A DPP please remove the maize cobs on your party cloth and send them to Admarc!
Billy Muyaya chonde auzeni a DPP kuti bodza silabwino
kodi a boma mukufuna anthu afe ndi njala chifukwa ciani inu osabvomera kuti chimanga mulibe kumanamiza anthe kuti muli ndi chimanga 50, 0000metre tonne koma liri bodza. chimangacho chirikuti anthu akufa ndi njala.Zitsiru inu a Chiyembekeza chifukwa chiani mukuuza anthu zaboza DPP ndi chipani cha utsiru.
The best way is to beg and be given and in situations like these when we have droughts and hunger companies will understand the problem and will help.