Email a copy of 'Wanderers 2-2 with Blue Eagles: Malawi TNM Super League' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

31 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Buyoya mawira
Buyoya mawira
8 years ago

Masapota a Wonderers ndiwo ma savage coz anaphesa munthu Ku balaka chifukwa cha ndeu, anayendesa ma players awo pansi Ku MZUZU, kuchosana pa udindo osasata constitution ya team. Usavage udutse APA.Zakukanikani matama thooooo.Mwayiwona Bangwe

chakuda
8 years ago

Zizayenda tym ikadzakwana

kulinga
kulinga
8 years ago

Neba wakhala ukuluza mbuyomu kufika pomanena kuti bola kusiya kusewera super league chifukwa mumasewera ma games ambiri. Ife sitimakunyozani chonchi. Anthu sanama akamanena kuti timuyi yachuluka masavage. Tisiyeni ife Manoma ndi Manoma. Tikudziwa kuti tsiku lina zidzatiyendera.

francina mbawa
francina mbawa
8 years ago

I love manoma for eva

Ziggy wa manoma
Ziggy wa manoma
8 years ago

Tili nayo nga,nga,nga noma ife

kangoma
kangoma
8 years ago

kodi mufuna adzachite kukuvoterani mu std cup

wanyerere ubooka mmimba

ehe chitimu chomvesa chisoni

The Lenzo Of Jickson
8 years ago

I Love Nama Mngakhale Sikuchita Bwino

Suzen
Suzen
8 years ago

Manoma oyeeee zivute zitani tili pa mbuyopo chi team cha anthu ozindikira ichooooo

mkalapwanasyo
mkalapwanasyo
8 years ago

Neba khala chete iwe cup watenga kale. Nyerere ndi Nyerere basi.

Read previous post:
HRCC censure Malawi Congress Party over racism attacks on MP Bisnowaty

The Human Rights Consultative Committee (HRCC) has asked Malawi Congress Party (MCP) to denounce insults and racist attacks its law...

Close