Email a copy of 'Wanderers to take part in Chief Minister’s Cup in India' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

34 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
MWEMBE
MWEMBE
7 years ago

Timu koma iyi, moti pano matimu M’Malawi muno ndi awiri basi : Number one Noma(Nyerere) mwana wake ndi Wizard. Amenewa ndamene amasewera mpira weniweni osati basketball ya Maule kumene chikagwere ndi komweko, ayi. A Ndudu/ Fodya BB taphunzirankoni mamenyedwe osati ngati gofu.

MWEMBE
MWEMBE
7 years ago

Jaffali Chande will join the team to India, outside Africa.Manoma woyee!!!!!!!!!

jester
jester
7 years ago

that’s my team

Thibho
7 years ago

That’s why i love you guys. I ‘ll never leave wanderers alone.

Johns Tembo
Johns Tembo
7 years ago

Nyerere tikukufunirani za bwino zonse. Uwu ndi mwai wanu ngati timu komanso ngati ma players. Kasonyezeni kuti ku Malawi anyamata aliko odziwa mpira. Kuchitabwino siwekha but a contribution of several the keeper, defenders, mid-fielder strikers ngakhalenso masapota, a coach ndi wena. Mukapeza mwayi agawireni anzanu osati nokhanokha. Tisachedwe kuloza zala anthu wena. Maso athu patsogolo. Tiyeni tiwone zoofoka zathu ndi ndi zotilimbikitsa. Pasakhale kukhomerelana apa. All the best -supporter wa Nyasa Bullets

KWEENI MPULOFETALE
KWEENI MPULOFETALE
7 years ago

The Wise People’s Choice…osangoti People’s ayi that is too General, But The “Wise”

Goliati
Goliati
7 years ago

More fire nyelele, tikakoke chikho chakuIDIA!!

josephynjovuyatopa
josephynjovuyatopa
7 years ago

GO KONKO GUYZ!!!!!!!!!!!!!!!!!

kambanizithe
7 years ago

Noma ndi more fire nsanje siumuna maule tifunireni zabwino inunsu Ku cap mumatibweretsera zoipa. Chaka cha mulungu chaloza komaso ubwino wake tikabwerako bwino opanda ngongole.

Alex Smart
Alex Smart
7 years ago

Abulets Ndi Anthu Oipa Kwambili Ngati Satana

Read previous post:
Malawi basketball league takes K50mil begging bowl to Bushiri

Central Zone Basketball League (Cezobal) has reached out to multimillionaire Malawian prophet based in South Africa, Shepherd Bushiri to help...

Close