Email a copy of 'You go! Chimodzi faces sack: Malawi FA call for emergency meet' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'You go! Chimodzi faces sack: Malawi FA call for emergency meet' to a friend
Former Justice Minister Ralph Kasambara triggered debate on social media when he challenged Malawi government through the NGO Board against...
Waziwona yekha chimoza amawona ndimasewera azawo akamakocha.
Chimozi ndi munthu wa sanje anamubisila mpeni kumphasa Kinnah . Amati atani iye bora kina anayesesa. Akudana ndi a tumbuka . Nanga Fisher player wabwino osapasa game . Chindere chakufikapo
A Chimodzi anamusemera chinyau Kinnah, I wo amaona ngati ndi zophweka. Izo alephera amati atani. Kinnah is one of the finest Malawian Coaches osati a Chimodzi. Ndiye likakuonatsoka amayamba ndi a kuba kulowa mnyamba mwako kenako ntchito ndikutha. Mayooooooooooooooo ineeeeeeeeeeeeeeeeeeeee!
Akalime basi kape ameneyu sizothatha matchansizo iya!!!,wabandabanda chamba chakaning’ina uko angakoche flames zoba ameneyu,zandinyansatu,kodi wakhungu angathe kutsogolera wakhungu nzake?CHIMODZI ndekuti chani?Zanzii Chancetakers are always accident makers ngati alibe khasu timubwereka akalime basi,wandikwiitsa kape ameneyu
Harawa and Malata no more 4 Flames…..!
Football is a game, Adakakhala Kina phiri Koma, coz experience counts when it comes to caoching,chimodi was nervous according to himself.
Malawi has wonderful players but grade 0 or 1 coaches probably biased living good legs
We have a useless goalkeeper, fire him not the coach.
Well done Zimbos. Keep whopping these flames boys till they figure out what they are trying to do ….
Kikikiki. Blame all losses onto the texhnical pannel, regardless of who exactly has to do the kicking of the ball into the right net on the right side of the field. If the swiftness to action and determination to move to the top that we see in football was transferres to politics, our parliament, capital hill and judiary would alreaways be on their toes, and someone would already be out of plot number 1 and front benches at the hero’s acre in Lilongwe.