Email a copy of 'ACB arrests Thuso Group’s Ganizani Kuchombo for money laundering' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'ACB arrests Thuso Group’s Ganizani Kuchombo for money laundering' to a friend
The Episcopal Conference of Malawi (ECM) has appointed Father. Dr. Henry Saindi as its new Secretary General. The 42 year...
Akulu awa ndakuba kuyambila kalekale ndimadziwa .. sizachilendo kugona mchitikosi…ali ku TNM anabanso awa…angokwanilitsa malemba apa..mufinyeni ameneyo…
Why is it that it has taken so long. Something must be wrong with the system. We started hearing or reading about thuso long time ago.
What about DPP gurus? What about 92 billion? What about Mulli? I hv never heard a politician arrested on Cashgate allegations why? Where is Khumbo Kachale? Stop arresting anawa timachange chabe iti, they were just used by our greedy politicians… This Cashgate thing could have been cleared if MCP was in power otherwise nothing tangible will be done bcoz DPP and PP are all children of a great thief UDF…
All department same
Kubaku sikudzatha mpaka yesu adzabwere kudzatiweluza basi.komabe tikuyembekezera zimenezo yense opezeka ndi ndalama zakuba agwidwe ndi kuimbidwa mulandu koma kungolekerera ndiye kuti tidzakhala ndi malawi wosokonekera.
Wadyako mbali yake musiyeni iyaaaaa
We want ACB to catch a big fish not these matemba we want bombe, shark, whale etc.
Stop arresting people,concentrate boosting economy please,we want work
Anaonerara akuluakulu ku DPP NDI KU PP basitu sanayambe yekha zonsezi pali anthu pakati apa fufuzani bwino otsathamngira msanga ku khoti.
My money my Tax, we are deducted lots of monies in what ever we do, and some pipo getting the monies without supplying goods or services. MaRubbish we sweating for these monies thats why I get reluctunt paying packing fee coz its all money wasted with poor and dirty roads. Asa am proud of malawi but not proud of malawians.