Email a copy of 'Kalonga, Katengeza found with case to answer: Malawi ‘cashgate’' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Kalonga, Katengeza found with case to answer: Malawi ‘cashgate’' to a friend
Staff at National Food Reserve Agency (NFRA) have started an indefinite strike over of workplace grievances, including demand for pay rise...
Its sad but prison is a very hard place. I wish there was another way for them to right their wrongs. We are all sinners and fall short of the glory of God.
Kalonga is a thief; his salary couldnt afford him buy a motorbike, but the chap was driving Range Rover and Merc. He should go to jail same like Mrs Senzani, who in fact stole less than him. Let this fool lot in jail
UKAKHALA NDI MILANDU, SUMAVUMERA AYI.
KOMA MLUNGU NDIYE AMENE AMAZIWA,NDI KUTHAZIZA KUWELUZA, TSOKA KWA AMENE AMAKANA ZOONA.
good
GYP and KK Propertys missing on the roads of Malawi! Those properties were acquired by Cash gate proceeds! Get them arrested even if they won’t return but they have to be in Prison! In three to four years time behind bars, life will never be the same! Ask Macholowe or late Kwacha Ghambi! Money will not set anybody free but truth will! All the thieves better surrender now because your days are numbered. You can delay justice but the hand of God will reach you where ever you hide!
Dr Ken Lipenga mulindimwayi koma moto ukubwera konko sizingatheke kuti inu musapezeke mugulu la kubalo chifukwa inuyo nthawiyo munali nduna ya yoona za ndalama.Mwasamba achimwene kuMulanje simasewera asambireni anzanuwo koma Mulungu akuona
Are you telling the nation that Dr Ken Lipenga is not involved in all these cases and yet he was a minister of finance in DPP and PP luring ? What about all those Fleet of KK Properties trucks which are not seen on the roads of Malawi are they parked or they have been exported to a neighbouring country ?
Koma kuweruza kwake kukuchedwa, kalonga ife tinamuyiwalatu. Koma akanakhala mphawi wopanda dzina bwenzi kalekale atatopa nako ku maula. Nanga Carol Savala-P ali kuti? mukamachedwetsa chonchi mukuwapatsa mpata womaliza ndalama zonse nde ngakhale akalangidwe sadzavutika akadzatuluka.
Penapakenso boma lathuli ndi lokondera.
Leonard is a thief by birth.
peter ndi getrude mutharika muwamanga liti pa nkhani za ndalama zomwe anapititsa ku mulakho ndi beam