Email a copy of 'Malawi court sticks to judicial review on MRA commissioner Namalomba' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi court sticks to judicial review on MRA commissioner Namalomba' to a friend
Head Coach for Mzuzu University football club popularly Alex Ngwira has advised Zodiak sports reporter Mike Bango to always strive...
edina kamoto
gogobawo! anthu ake ati? ife we are not complaining aboit shad, ndipo titolela bwabasi koma kamoto yekhayu achokepo honestly
game nkuza tembenuka pamene paja, mra pliz tikufuna chilungamu chankhaniyi nsanga yatitopetsa ngati kuli kubwenzera namalomba pa ntchitoyo chitani nsanga coz kutolela makobili kwayima tiyamba kudanaula pompano kuti sitina tolele bwino
Roza Mbilizi, Shad Namalomba and Kamoto bwana Peter Mutharika achotseni awa onse ku Mra. Roza ndi Namalomba akupanga campaign mseli kufuna kumugwetsa Kamoto. Koma bwana President musadzayerekeze kuika Roza pa udindo umenewo mudzaonanso no revenue colection. PEMPHO anthuwa onse atatu achotseni na ngati muli ndalangizi abwino am one of them coz zinthuo ife tikuziona ndithu. ndi mmene zililimu anthu agwira bwa. Anthutu agawanikana nde piliz thandizani MRA pochotsa anthu atatuwa tumiAnkoni a mulhako ena aliko ndithu ngati mufuna milhako yanuyo
Nansongole uyu. Abuse of power.kunditukumula uyu. Usova
Thom Main ganja mus resign now. Bring back Bisiwick. Ralph is a failure.
Thom Mpingangora must resign. If not no tax revenues will be collected. Bring back Bisiwick take this fool back to Mera
Kamoto matchaba ako. Ife a lomwe tithananawe tipatse time we are removing u from MRA.
kenyata nyirenda nzozodo amwene akanena wanena ask PP and MCP gurus za judge ameneyu amamva naye madzi.
Kkkkkkkk game tembenu, all of you should follow the procedures, should not act emmotionally.