Email a copy of 'Malawi Police shoot, kill armed robbery suspects' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Malawi Police shoot, kill armed robbery suspects' to a friend
The Public Affairs Committee (PAC), an inter-faith organization comprising main protestant, Catholic and Muslim faith groups in Malawi has said...
good pa good.muziombela pa mimba mabwana
Mukagwira mbava ipheni
The moment these robbers have guns and pangas,just know that they are coming to get somebody’s life.So the police do not need to have mercy with them.The only language they understand is blowing out their filthy brains from their useless heads.Finish them all.We need a Crime Free Malawi even the outsiders coming to cause havoc in Malawi will be doing at owners risk.
Thumbs to the Police.These Lowlife Scum were there to snuff out mercilessly somebody life if not discovered earlier by police.Good that the police are getting rid of these scum who are always thinking of making easy money.We need a clean Lilongwe.Shoot them all like pigs.Amatibowa muma location umu ndi makobili okuba surrounded by money hungry bitches.Tikufuna kuti mtsogolo umu ttizizayenda 12 midnight with no hassles like in Kigali.Mulinso ana amabwana okuba ndi mifuti muma area umu nawonso akapezeka just get rid them like chicken.There are parents who doesn’t ask their children where they get different stuff without having proper source… Read more »
Shoot to kill policy ? Mbava ziyamba kuwopa tsopano
Congrats police. This isa what peace loving Malawians have been asking for. Of course where possible, as you have done in this cxase, arrest one or two so that they can devulge reveal details about their accomplices both dead and living. Once again keep it up. Anyone who criticises this is an enemy of peace loving Malawians and is a potential accomplice
Koma abale mukumuonetsetsa mkuluyo ziwalo zake zitalizitali. Ameneyo kuti wakulowera mnyumba basitu kumangodzikodzera ndi mantha. Komanso sangakusiyire moyo uyu. Ayi Mulungu wayankha apa.
Ndimati ndingobenthulako pang’ono kuti midzi yonse yomwe yazungulira mzinda wa Lilongwe ndi ma safe haven a mbava zoopsa. Tsiku lina mudzangokhala ngati mwachita chipikisheni mudzaona anthu ogona masana kukonzekera move usiku.
Zikomo kwambiri inu a POLICE athu pa kankhani kabwino chonchika. Pempho kwa a Malawi anzanga amene muli ndi kuthekekera mukhoza kukonza ka mphatso kapadera kwa a Police amene agwira chintchito cholemetsa koma chotamandika choterechi. Iyi ikhala ngati incentive. Kuyambira lero inu a POLICE ndife pachibale mwamva!
No mercy with these guys once they find you in the house, they sometimes hit you to kill in order for them to instill fear in you so that you give them what they want. They deserve stiff punishment though the best would have been to disable them as oppose to kill instantly. If disabled, they may pose a good lesson to others would be perpetrators/offenders.