Email a copy of 'Miss Malawi to be crowned tonight: 14 beauty queens to contest' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

11 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
lesley
lesley
6 years ago

Gladys Kumbatira is not growing. In October, 2011 when she was dating Mnthumwi Pisky, she was 20 years old while studying at MCA, six years later she has only added 4 years. Koma yaaaaaaa!

pixy
pixy
6 years ago

Amenewa ndiye mukuti akazi okongola ,kaya mphanda zinazi ndiye mwazitenga kuti.munthu kuonekeratu pojoina myendo looo !!jamani !!!! mbala sizingavutike ndi anthu ngati amenewa ma expand awo ndi otsegulatsegula kale No problem .

Ronnex Makuluni
Ronnex Makuluni
6 years ago

All the best, let the best of the best carry the day

marshall
marshall
6 years ago

kod akazi okongola ku malawi kuno anawaletsa kupikisana nawo pa uchiphadzuwa wa kuno ku malawi ? zimandidabwitsa kuti akazi omwe amapikisana nawo samakwanila kukhala miss malawi. zoona matupi amenewa azungu aziti ku malawi kuli njala yosatha ya mgonagona ndiye bolanso kutenga anyani azipikasana akhoza kumakopa alendo langa ndi pempho muganizilepo bwino

chilombo
chilombo
6 years ago

CV ya Nthanda ndiyowinawina kale 90% kwangotsala 10% yoti akokele ndima looks,catwalking and speech. I’M FOR YOU

kate
kate
6 years ago

Competition is btwn yvonne n thanda ……

Colonel Gaddafi
Colonel Gaddafi
6 years ago

Akuchitani ndithu

Le Cologne
Le Cologne
6 years ago

Koma ku Malawi komvetsa chisoni ndithu. So these skinny shabby looking girls consider themselves beautiful? Pitani mukaone pa Nairobi, Maputo, South Africa, Addis Ababa ndi Lusaka.

chilombo
chilombo
6 years ago
Reply to  Le Cologne

@Le Cologne – Ndiye ukufuna akazi aku Nairobi, Maputo akowo azakhale miss Malawi? I bet if you have a girlfriend/wife, she is Malawian kkkkkk unagwira onyansa!!

Bauleni Makawa
6 years ago
Reply to  Le Cologne

Akulu pathako panu…..Kuno ndikuMalawi!! Zakumazambiki zanuzo kagwele nazoni uko!!! Ife zathu ndizimenezizi….asafuna asiye

abby
6 years ago
Reply to  Le Cologne

anthu samakhala ofanana brother,

Read previous post:
Malawi govt denies ‘Lhomwelisation’ and nepostim accusation:  Dausi hits at ‘apostles of misinformation’

Minister of Information and Communications Technology Nicholas Dausi has denied accusations by a group of civil society organisations (CSOs)  that President...

Close