Email a copy of 'No ‘tractorgate’, Minister clears mist on 177 tractors from India' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'No ‘tractorgate’, Minister clears mist on 177 tractors from India' to a friend
Football Association of Malawi (FAM) hottest presidential contender marketer-cum banker, Wilkins Mijiga has officially launched his manifesto outlining his vision...
@Ben, very good and valid point. That’s what we call simple uncomplicated economics. The government are so dumb such that they can’t see that the decrease in value of the Kwacha is having a massive negative impact on farmers . The fact that the farm inputs are acquired at such a high value in dollar terms than the selling value of the produce, it is a naked truth the farmers are at a disadvantage. This country is being governed by people who have got to no clue. What’s going on? Look at the new president of Tanzania and the Rwandan… Read more »
Kamlepo amakhala ndi umboni all the time koma samaunena.amangoopseza basi,to be honest I think he is a joke amangontenga nkhani zomwe amakamba ndi azimzake ku bala ndikumakazinena mu nyumba ya malamulo kkkkkkkkkkk
The truth of the matter is that Bingu took some of the tractors to his farm, period. Some districts did not receive the allocated number of tractors and were told that it was the direction from above. So, Kamplepo is right and he might indeed have the information as evidence. Check. with file number ……………. at capital hill (min of agriculture)
If this went according to procedure, then why am I not aware?
How was this advertised?
What was the basis of selection?
This is not acceptable by any standard.
Zambiri tizimva apa mpang’ono palibe chinsinsi padziko lapansi lino,muziwe zimenezo.
where were you yesterday when the Mp was asking you in your own ministry? ndimamva chisoni ndikamadutsa kumudzi kwanu a Chiyembekeza kodi anthu akwanufe sitimafuna nseu wabwino?? undiyankhe ndikudikila
Muchiteni corner Kamlepoyo apeleke umboni umene amanenawo kuti ali nawo.
u leader of opposition akanati azivota kunja kuno osati set rules Kamlepo unatenga vote yanga, ya mkazi wanga, ana anga,makolo anga, makolo a mkazi wanga ndi ena ambili ndamvela ma comment a onsewo oti ku opposition kulibe wa nzelu ngati Kamlepo awo a Chakwera khaya mukuti Chatsika maso awo ali pa 2019 basi ‘electrol laws’ thats all he know. How do u expect to win wthout a single constituency governor n the north & south achitsilu inu kkkkkkkkkk awa! tulo basi
Mmmmmmmm kaya mwina chilungamo chonse akuchidziwa ndi Mulungu.
Procedures no procedures, is the government in the business of acquiring tractors on loan on behalf of poor Malawian rural farmers and then sell them to undeserving rich Malawians? Why kulemerera pa anthu osauka? Mulungu akukanthani muona, chaka chake ndi 2016! Ma…nde amu nonse. By the way, who will pay back ths tractor loan?