Email a copy of 'Wadi says don't blame President for poor Malawi economy' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Wadi says don't blame President for poor Malawi economy' to a friend
Former Nyasa Big Bullets General Secretary, Higger Mkandawire, has expressed worry over the confusion at the club. Following a misunderstanding...
A Wadi tamangophwisani muliko palibe amene angakutolenkoniso
Malawi is full of corruption, high expenses, poor in economy, low wages of salaries, come and see rural areas people is suffering, you are talking as you don’t have knowledge at all, dot look the way you survive look at your colleagues they are suffering, government have more money but the management is very poor in mind they don’t look at people how they are surviving, employees paid poor salaries even private sectors, private sectors paid their employees k20000 the government just pleased with it, my friend poor in your thinking capacity.
Wadi wadi wadi!!!!!ukuoneka kuti zakyvuta uli biiii ngati wolisha ng.ombe sizikukuyendeera they say desparate person will land at anything that appears helping this is t wadi you’re desperate for your own affairs you will not taste heaven we will leave you here with your fellow satanas
Go to hel….due to that (corruption) t-chaz r nt paid….the day will come and he gona realise
KOKOROCHI UYU ANALI KUTI NDIPO AKUFUNA CHANI MBEWA AMENEYU? ANAKUTHAMANGISA BINGU NDIYE UKUYESA KHALAMBA YAKOYI IKUTOLA HEHEHHEHEHEHE ICHOOOOOOOOOO!!!!!!!!!
Mmmxxxieww!!! Mmmh!! Malawi, ka dziko kovetsa chisoni,kadziko kamene anthu ambiri omwe anaphuzira mmitu mwawo munangodzadza mamina,mikodzo even manyi ndithu,look amene mukuti ma Dr,ma professors zimene akulipanga dziko lino?zovetsa chisoni,anthu amene sanaphuzire ndi amene ali patsogolo kutukula dziko lino with different businesses podula misonkho while anthu amene akuti ophuzirawo abisala mma office kumaba ndalam za anthu amene akuvutika kugwira ntchito..mbatama zophuzira destroying Malawi,shaaaaaameeeeee!!!!
Together we can build malawi..poor minds ndiye vuto….wadi your right,,i totaly agree you
How as citizens, can we build malawi together ?
As the Malawian we don’t want APM anymore everything were happening bcz of his poor administration failing to run our nation !!!!!pa atsogolire wose amene takhalapo nawo koma uyu walephera
fodya kkkk eti a wadi kkkk walemba mmadzi
Koma kumeneko!!!! But there!!! Repositioning…..kkkkk kupalira tsopano. Ukuitha man. For the first time kuona venda akutchipisa maize than ADMARC. A lawyer akuti zili bwino.