Email a copy of 'Zulu quits as PP deputy secretary general, joins MCP' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Zulu quits as PP deputy secretary general, joins MCP' to a friend
When the Vipya sank 68 years ago, killing nearly 150 of the people aboard the ship, one person the tragedy...
power-hungry man will always be a rolling stone. musiye tukumutukumu
Vuto lanu bambo zulu ndimaziwa kuti gule simungasiye.mbalame zofana nthenga zimawulukira limozi.ndinu omasuka kavineni bwino gule wanuzikomo bambo.
Welcome Zulu!! Mcp is in your blood. My advice is avoid being emotional otherwise mupweteketsa abale anu. Auzeni anzanu abwerere msanga bwanji wuyimbira mmanja gule wa eniake.
nepotism mwayiona liti? Best and satisfactory reason would be the running away of your leader from the country following her theft revelation period
CHonde Bambo Zulu, bwerani ku chipani chanu cha PP chomwe inu munatisimikizira pamaaso pa Amayi kuti simudzawasiya, simudzawataya kapena kuwathawa koma kuti mudzaima nawo nganga mpaka mmanda. Nanga lero zataninso. Pitani inu ndi a Msonda muzikafuula kuti ” Pipipipi! Odii ukoooo! Amayi adutse! muwayitanenso Amayi kuti abwereke kumene akubisalako. Kodi si aja ankatiuza kuti dziko lino ndi anthu ake iwo amalikonda ndipo sangachoke mdziko muno kusiya anthu awo akulira? Abwereko basi ngati ankanendadi kuchokera pansi pa mtima.
its not time to comment on political issues….Mulungu dalisani Malawi wathuyi.
keep it peaceful and stable. Holly ghost fire kwa oyipayo…
Good bye Zulu boy sorry you have gone with a thin wallet and don’t think chakwera will offer you a fat wallet. You’ve been a fat chancer! Maybe try your luck with Edgar Lungu next door!
Mbalame yabwerera kuchisa. Tiyeni tikonzeso dzikoli abale. Zipani zones zomwe zayendetsa dzikoli kuyambira 1994 zaononga momvetsa chisoni. M’Malawi wanzeru zoongoka ayenera kubwerera ku MCP.
How can one be opportunistic for leaving one opposition party to to another? If he had gone to the ruling party, that argument would have made sense. A malawi lekani talking trash all the time about people. If you are worth any salt, why dont you join the politics yourselves to do better? Welcome back to MPC bwana Zulu.
Good Decision George Zulu. MCP needs to regroup and close down the central region from the other parties and the time to get started is now. I know George was one of those who pushed for leadership change in MCP after 2009 and he left because he was expelled. Welcome back home to the mighty MCP – we need your energy in the Tambala party.