Email a copy of '298 000 pupils begin primary school leaving certificate exams' to a friend
Loading ...
Email a copy of '298 000 pupils begin primary school leaving certificate exams' to a friend
Former main opposition in parliament, the Malawi Congress Party (MCP) says it will not take part in peace prayers which...
DPP government has failed in all areas but this is too much.
zochititsa manyazi kut zinthu ngati zimenezi zikuchitika munthawi ya ulamuliro wa A mutharika omwe adaphunzitsapo maiko ambiri komanso amadziwa bwino lomwe kufunika kokhala ndi zipangizo zomwe zingagwiritsidwe ntchito polemba mayeso
A Malawi ife ndi anthu omvetsa chisoni. Tinali ndi Kamuzu amazunza ndiye anapita, Demokalase inabwera koma siikutithandiza ata. Tikuvotera anthu oti olephera. Peter Mutharika olephera kuyendetsa ministry, AMalawi ndikumupatsa kuti ayendetse dziko lero ndiizi zinthu zingopita pansi. Education, Corruption, Nepotism, Tribalism, Poor Roads contructed by one company the whole country, Mota Engil. Kaya kulibe ma company ena kaya? Ndiye muvoteranso yemweyo wolepherayo, wa kubayo! Ndi muziliranso. Zanu zimenezo.
And idiot Atupele thinks he can give them laptops. Stupid. Give these pupils chairs and desks..
Eya writing exams sitting on the floor APM is developing Malawi like UK or like USA ndithu crying to be given another term zandowe basi.
Students sitting on the floor in 2019. This 55 years after independence and 25 years after gaining democracy. What a shame to Malawi. Photos like this one should make us swallow our pride, we should be angry for change, we should be sad. This is exactly what I went through between 1976 and 1980. And yet still 40 years later the situation remains desperate. Hi here is the development DPP are boasting about? Why should the parents of these children be denied their vote because somebody rigged elections? APM and SCK you have raped this country for nothing. This time… Read more »
I cry for my girl sitting on the floor, the one in blue shoes. Can she solve maths in that position? Can she concentrate on the paper having in mind that she has also to mind her dress from falling off the tacking. Yet she is expected to compete with those sitting for the same exam in cities. oooh my GOD!
Minister of education where are you? Mumapereka ma desk ku machinga nanga uku? Your boss is busy telling Malawians that he has transformed Malawi. Is this what you call transformation?
Nde mpinganjila blown akunyadila kuima paculu. Waiwala nthawi ya UDF anatebga donation ya mmasukulu ma copy etc kugulitsa ngati kuti zinali personal property. Muluzi kept quite kupeleka ulemu poti kwathu kuno system ikuoneka kuti ikienda ndiyosamumanga munthu akalakwa but high in ma commisoon bit no verdict. What a waste of money.
And we want tupele awino tate wake azimupopera kumbuyo.etini
Kodi zogula ma material, ndalama zake nzakutiko? This is too much toooo much waste of money. abd i can assure pipo kuti makolo ena akongola ndalama olo anawa kucititsa ganyu ya zolembela. Trust me. And here they are splashing money buying party regalias now competing in show bizing. Mpakana ma blue wig omwe amavala ma supporter ampila ku Ireland why not donating the money to develop our country than these single used materials like condoms. My mother Malawi. Now ma ballot papers aabwera eti. Wina asaelekeze kucita tampet. Muone mmene titamusololele matumbo fromthe backside. He will receive the briberd money… Read more »