JB’s sister Cecilia Kumpukwe arrested

Malawi Police in Blantyre on Tuesday morning arrested Cecelia Kumpukwe, sister to former president Joyce Banda.

Details of her arrest, including charges are still sketchy but the police are taking her to Lilongwe where Stella Asani, suspected to have authored the  fake resignation letter of vice president Saulos Chilima is being kept.

Kumpukwe: Arrested

Our sources say Mrs Kumpukwe may have been part of the syndicate that plotted to write the letter.

Asani has not yet been charged although she has been in custody five days now.

The police also say they are looking for Ackson Kalaile Banda, another Peoples Party official.

Police spokesperson James Kadadzera says he has not been briefed on the arrest of the former president’s sister.

Mrs Joyce Banda has been in self imposed exile since she lost the presidency in 2014 to the incubent Peter Mutharika.

Follow and Subscribe Nyasa TV :
Follow us in Twitter

31 replies on “JB’s sister Cecilia Kumpukwe arrested”

  1. Kuchititsa manyazi boma la DPP. Konsekutu kusonyeza kusowa mtendere ndi kusabwera kwa JB. Amai amakuopani muzikhala ndi confidence

  2. Kodi mukamaloza munthu ndi dzanja lanu, ndizala zingati mumamuloza nazo? Nanga ndi zala zingati ziloza inu? God is watching. Freedom is coming tomorrow.

  3. In this forum grammar does not count. What matters is content. You have already understood the other person wanted to say. Stolen or stolen, Chaponda ndi wakuba basi

  4. Those who believe, let us pray that God intervenes in anyway as long as Malawians get their freedom. Amen.

  5. kkkkkkkkkkkjk munyera agalu inu mukudana ndi alhomwe. these are two different issues, unless you know something that maybe chaponda had something to do with a fake resignation letter then yes ngwengwengwe for his arrest. Chaponda paid for his stupid actions, as we both know that he is no longer a minister. Nawenso abit pakunya pako. ukungoona ngati mulungu ndichoopsezela anthu.

  6. Political persecution. When shall the mother Malawi be free from this stupid, sticking politics of bwampini and his group of thugs Deaf Progressive Party, the more u persecute the more this patty un popular. May God free us from these devils.

  7. kkkk….ndale pa Malawi, wopha anzawo sanapezeke mpaka piano koma wolemba kalata za fake nde kalekale mwagwira??

  8. Chiyembekezo ndiri nacho mwa Mulungu wanga. Wotisamala Mbuye, sagona tulo ai sadzatisiya tokha. Chimwemwe chidza kummawa. God show Malawi that you a caring Father. Amen

  9. Let truth prevail..enanu mumangopanga comment zinthu zosiya ndi nkhani apa..kodi mukamapanga defend some well to do people nde kuti unyolo anapangira amphawife? Ochita bwinowo ngotetezedwa? Iyaaaaa.. Do you know how many poor people are being arrested daily for various crimes…aaaaaaaa. Sober up guys….relevant comments plz..

  10. Nyansa times are you sure with your reporting. I t has been announced on Radio Fm that this is not true.
    Go back and check again

  11. Komatu mnzanuyo akupweteketsani. Iye alipheee kunjaku akungotuma inu zopusazo. Wosamuuza abwere azidzapanga yekha bwanji? Bomatu silosewera nalo ayi. Take example on how PAC’s leadership is now shrinking. Abale tadikirani nthawi ya chisankho mudzayese ngati anthu akukufunaninso after throwing you to number 3.

  12. Komatu Osamayiwala nsanga. Kunja kuno kuli Mulungu osamamuyesa akakwiya amapanga zoopya. Mulingo omwe mumamuyesela nzako ndi omwe mulungu amakuyesela.

  13. Osamanga kaye mlomwe mzanu uyu mukuti Chapondayu bwanji? kodi mufuna tonse tikhale alomwe kuti tisamamangidwe ——- koma chilomwe vuto lake ndichovuta kuchiphunzira — ngakhale bwampini sangachikwanitse——kkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkkk—- mwafikapotu, alomwe dziko ndi lanu basi.

  14. Why is Chaponda not being arresyed? Is it because he was stealing together with other important people

  15. THIS IS STUPID , CHAPONDA STEALD ALOT OF MONEY TU BE PAID BY POOR PEOPLE TAXES, BUT NO ARREST HAS BEEN DONE KODI INU ADPP MUMAYIWARA NSANGA ETI Mikuwona ngati mwafika ,its just amatter of time.

  16. Dangerous times: if you are anything other than DPP, you risk your freedom. Why no charges after 5 days in custody?

  17. Zupita kwina zinthu zija……….
    Anyway, political things………..
    .
    .
    .
    .
    Mpaka chilungamo chionekaaaaaaaa apolisi athu sapita pachabe.

Comments are closed.