Email a copy of 'Admarc board sends Mulumbe on forced leave over ‘maizegate’: Mauwa acting CEO' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

31 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
wenecho
wenecho
7 years ago

DPP = DEAL PAFUPI PAFUPI
HEEEEEEEEEEEEEEEEEEE ALOMWE ALOMWE

Kusolola
Kusolola
7 years ago

I see that the ADMARC Board is showing much better leadership that our president. Kodi munatontenga kwayani ameneyi? Koma atotikwana bwanji. Asaaaaaa.

lomwe
7 years ago

Mr president could you please suspend Chaponda otherwise apa a Malawi tiziti izi nzogwilizana nonse ndinu mbava.We are tired of DPP Govt.full of thieves.

Patriach
Patriach
7 years ago

Tsopano Ndiye Nayenso Chaponda apitetu ku forced Leave Nanga kungomuthothola Mulumbe basi. Mafiozo nayenso athotholedwe.

Lover of life
7 years ago

Time alone will tell. Dzikoli ndi anthu ake mzaYehova wamakamu.

che nnungu
che nnungu
7 years ago

Galu wakuba weniweni ndi Chaponda. Nayenso achoke to pave way for investigations. Ngati amaganiza zoti adzalamula Malawi achotsele. Akalamulila kwawo konko. President samakhala wonyansa chonchija. Kunyansa nkhope, maganizo, chilichonse

Kwayipa
Kwayipa
7 years ago

Let this big fish also go on leave, why are you shielding him? Am asking Mr.
President.

Thinktank
Thinktank
7 years ago

Chaponda and mutharika are in the same boat…of stealing from government coffers. ….

mary
7 years ago

No no no no mtsamilo uwu! Chaponda achoke!
Zinazo mbuyo!

Chancy
Chancy
7 years ago

APM & Chapponda ayudas enieni a dziko la Malawi. Anaba mavoti pano akupitiliranazo. God sees u.

Pida
Pida
7 years ago
Reply to  Chancy

KOMA PAMENEPO ACHIMWENE MWANENE ZOONA ZEDI

Read previous post:
DPP Kachale tells court prosecution will prove PP scheme in ‘Cashgate’ and Mphwiyo’s  mastermind role

Director of Public Prosecutions (DPP) Mary Kachale has said the prosecution will prove its case on how  Cashgate was schemed...

Close