Email a copy of 'Atupele says UDF strengthening to move Malawi forward: Malindi ‘thank you’ rally draws masses' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Atupele says UDF strengthening to move Malawi forward: Malindi ‘thank you’ rally draws masses' to a friend
Minister of Information and Communications Technology Nicholas Dausi has asked for patience on the operationisation of the Access to Information...
Thanks Nyasatimes for reporting that udf had 93 seats and now only 14. Kwinaku atsala ndi makhansala omwewo. Chiwaya wawona kuti basi the udf is in ICU on oxygen. Kutha ngati nsalu ya makatani. What is the point of sticking dpp? Are you not scared MCP managed 1000 votes? Shithole Atupele and shithole dpp. Chipatala chapsatu.
Congress guys very interested to comment about UDF issues kkkkkkkkkkkkkkkk.
Galu ulila dpp is playing a game on u Mia walowa kumeneko mcp 1008 votes
Atupele usanamize anthu a ku Mangochi kuti udzawina chisankho, wachepa nazo ndale, UDF ku central region ndi ku Northern region inatha kale kale, ku mwerako idatsala ku Mangochi ndi ku Machinga basi, komanso MCP yalowako through Mia, ngakhale mupange alliance ndi DPP, anthu akupanga zomuika Chakwera ndi Mia m’boma .DPP ndi UDF ndi zipani za ku banja ndipo zatha ngati makatani . Ndimakumbukila mawu a Bingu oti UDF waitha yekha Bakili anayithadi, pano DPP waitha yekha Pitala . There is too much Hurricane blowing in UDF & DPP . Now Atupele can’t be considered for runningmate to Pitala, Chilima too,… Read more »
UDF is a party for Mangochi , Machinga, Balaka and some parts of Zomba. The big win in Malindi is because DPP did not contest and its supporters managed to vote for UDF.
This is a direct reaction to Callista detonation. Atupere now realises he is a political victim, & with DPP squabbles he will end up being used like a condom. But its too late, Malawians have realised youre unprincipled just as the old politicians. Kumakidwa ma vote in your own backyard.
Mukazatoluzaso basi wa ku Boma .Kuthawa ntchito yanu yosusa.Onani telemu yoyamba ya Bingu zinthu zinayenda chifukwa Osusa anali ambiirri .Mnyamata ngati Iwe kukana 50+1.
He is a sell out. What a selfish man!
A confused boy Madhala GG @82 was referring to. People of Mangochi, don’t be betrayed by chameleons.
Amangwetu, Adyu mwanachedyu tachisumisya UDF dyi. Ngaaakunda awa. Ana welewa ali ku DPP kapena ku UDF?
WE NEED SIR LUCIUS BANDA!
No comment here but if it were DPP then you could have said you want young generation. Atupele is young so if you want a young leader vote for him. Leave DPP alone. Leave our mulupale alone. You have many choices to make. The people will decide their choice