Email a copy of 'Balaka man gets 7-years behind bars for burglary' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Balaka man gets 7-years behind bars for burglary' to a friend
High Court judge Dingiswayo Madise has told Kaporo Stars FC that the club violated rules of the game by taking...
Ameneyu amafunika life n prison wakuba ndiwakuphanso chisatuluke chigawenga ichi stupid judge
Waiphula, 7yrs kukadya zaulele. Anyamata aku balaka asamala nkazi Wako usadandaule.
Mudziwe kuti athu aku Balaka ambili ndi obwela ku chokela madela ambili. Why? Ambili anasamukila ku Balaka chifukwa cha chipAtala cha khate pa Utale 2. Read history ya Utale. Pano ndiye Atumbukaaaa Ali pose ponse. Mtundu uli onse uli pa Balaka. It is tribe less district. So do not ship where you eat.
All evil things are done in Balaka.They always look for quick riches.Sukulu ndi mpongozi.Kodi mtundu wanji wa anthu umenewu?
Its nice that the police hv arrested this thief and the keys should be thrown away.
Kungozuka mmamawa odabwa and obalalika
Balaka ndi no 1 asafuna asiye.
Mwera wavuta ndi maluzi
Kodi inu anthu aku Balaka tidzingomvela inuyo? Tsiku losatha koma zili ku BALAKA. Mwawonjeza mwamva.
M’MWERA AT ITS BEST