Email a copy of 'Chakwera, Mia  say MCP ready to take over govt: Promise better lives for the people of Malawi' to a friend

* Required Field






Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.



Separate multiple entries with a comma. Maximum 5 entries.


E-Mail Image Verification

Loading ... Loading ...

Sharing is caring!

14 Comments
newest
oldest most voted
Inline Feedbacks
View all comments
Sanga
5 years ago

Heeeede inu a MCP anthu anasowa kopita nangoti tiyese Congress chifukwa choboweka ndi DPP. Iyayi kwabwela muwomboli UTM moto buuu.leloso tiziti kwachaaaa!!zinapita kuwakufwa

Central
Central
5 years ago
Reply to  Sanga

Kwanu komweko nawe iwe, nanga UTM ku Dowa? Awanso! Koma Dowa umayidziwa iweyo pa nkhani za kongelesi!! Ukamufunse Kweni akuuzaaaaaaaaaaaa! Ndiyetu ovota aliko 325,062 ndipo awa ndi amene analembetsa! Titati tingochotselapo ka 5,000 ka pamwambako for null and void votes, muli m’madzi!! Nanga popeza NA, CK ndi Mangochi komanso MJ kum’mwelako kwalowedwa, kayaaaaaaaaaaaaaaa timva posachedwapa kuti anthu atatu cardiac yavuta, please ndege ikhale ready!! Dziwani izi, first 14 days onse ukhudzidwa ndi nkhani zosokoneza makobili athu ngati K145m adzakhala mukukawaonela pa bowo la waya ku maula ndithudiiiiiiiiiiiiiiiiiiii Ndipo kulibenso zoti iyayi ndi okalamba achitileni chisoni iyayi, mwaphetsa anthu anyani inu… Read more »

kuchekuche
kuchekuche
5 years ago

Anthuwa alibe mfundo. Kumvetsera zimene amayankhula eish sizamandifikapo ayi. Kodi manifesto ya MCP imati bwanji?

Central
Central
5 years ago
Reply to  kuchekuche

You remind me one thing I have ever encountered before! Just after a physics class, while some students appreciate the topic covered, others went out as they came in! kikikikikikikiki Kuchekuche are you serious the clip has nothing from MCP? Koma kumeneko, nzeru izo nzeru izooooooooooooooo

mtete
mtete
5 years ago

For the DPP zealots (including APM) who keep accusing Chakwera that he keeps criticising government but offers no alternatives, please carefully read this clip. You will find the MCP leader and his deputy has briefly outlined what they will do after taking over government next May. We only hope DPP will not elaborate the same issues during their poorly attended meetings. We hope we will not include MCP strategies in their next manifesto. DPP are well known for stealing ideas. Remember the UTM’s 1million jobs to be created once SKC takes over government? DPP produced their own version soon after.… Read more »

Zabura
Zabura
5 years ago

I like and love Chimwendo constructive ideas koma pano my friend is losing track too emotion .Just say mfundo osati attacking .Try ndale za chilendo

Point of View
Point of View
5 years ago

Kum’mwela akuti alinawo awawo maliseche, if pakati tikut tilinaye wathu mtsogoleri. 2019 Chakwera Boma

Zabura
Zabura
5 years ago

Lets be realistic anthuwa mfundo alibe .Mia mmene wayambira am a performer za 2013 eish mfundo tatulutsani.Chakwera kwathu ndi kuno Dowa ndi ku Mchinji amayi anga abambo anga pali mfundo nanga apa. Tiyeni anthu tiwawuze mfundo

Opinion
Opinion
5 years ago

This is what we want visibility is important. Go to the people and talk to them.

Chakwera Chingatsiketu
Chakwera Chingatsiketu
5 years ago

Let’s suppose that MCP wins. Its reign will be dominated by fighting between Chakwera and Mia – just like it’s always been between a President and his vice, but this battle will start earlier in their tenure. They are both alpha males (read okula mitima) and it’s an unholy alliance. Both have got different agendas concerning the reasons they decided to team up. Atambala awiri salira khola limodzi…MARK MY WORDS!!!

Wiseman
Wiseman
5 years ago

Tsoka ilo maso athu sakuona, bad combination.

Bystander
Bystander
5 years ago

Za Malawi Defense Force so mwabera SKC. He started it in Dedza. How do you manage concession tickets in today’s mode of transport? Today, unlike in the eighties, we have minibuses motorcycle cycle kabaza.

Salayi
5 years ago

Kkkkkk, MCP yikulota zolowa muboma,kikiki anthu anayiwala za kwacha!! Mucha cha 1994,lero tiyambileso zamake zana zoti kwacha!!. A MCP mazi akathika athika basi zoti MCP yizalamulileso a Malawi analumbila mu 1994. MCP yinapita, UDF yinapita, PP yinapita ndipo DPP nayonso yili pa ulendo, pa a Malawi akufuna kuwona za chilendo.

Truth Be Told
Truth Be Told
5 years ago
Reply to  Salayi

Wait and see. You are not the decider. You will be shocked big time. MCP is a silent killer. You will be shocked with the real landslide. The MCP voters speak in soft voices in the closets of their home. Travel from Mpemba to Nsanje Boma. Travel also from Jenda to Karonga through Rumphi. You will be shocked.

Read previous post:
CCAP Livingstonia Synod hails Mutharika for Njakwa-Livingstonia Road

The University of Livingstonia (Unilia) of the CCAP Livingstonia Synod on Saturday hailed government for constructing Njakwa-Livingstonia Road in Rumphi...

Close