Email a copy of 'Civo threaten to drag Linje to court: Accusing players of ‘theft by trick’' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Civo threaten to drag Linje to court: Accusing players of ‘theft by trick’' to a friend
Malawi government has organised “an open forum” on Monday 22 June, 2015 in Lilongwe where a cross section of people...
Aaaah! Tadziwa nawotu apa.
ameneyo ndi mbava ayenera kumangidwa basi kuti ena atengerepo phunziro.Rashid ndiwe wanzeru kwambiri.Ndalamazo abweze apo bi kundende
MHH
Eeeeeeeeeee! Km manom kundimvesa kukoma kaya neabour ukumva bwa?
ngat zampira smuzitsata zingoonerani ma film a chichewa omwewo.nkhani apa yagona pakut anasainira civo koma wathawako.ukamasaina pamakhala ndalama yosainirayo(signing on fee).sikut anali katangaleso ayi nd malamulo ake.bwanj Atsu wathawa ku MBW chifukwa chot sanamumalizre ndalama yosainira contract?Linje aona zokhoma ndithu naa ngati anasainirad contract n bfw iluza ma points
Hahaha za mpira sizipita ku court or mutatani mutani
Kani mumkapasa ziphuphu player? Nafe tiyiwuza ACB iwunikepo apo
Adachita bwino! Ntchito yanji yopanda ma dhinkamu?
Ndiwakuba ameneyo amangidwe basi 🙁
Is his choice let him go