Email a copy of 'Comedians Kansiime, Chaponda to peform in Malawi together' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Comedians Kansiime, Chaponda to peform in Malawi together' to a friend
Malawi has slipped to position 19 from 18 out of 54 African nations on the Mo Ibrahim Foundation (MIF) Governance...
Sichoncho akulu. Uwu mukuchitawu nde ndiubulutu ndi usatana weniweni. Asiye moyo coz of kuyipa kwa bambo ake? Uyu ndi Dalitso Chaponda osati George Chaponda. Inuyo makolo anu anali angelo? Ayi, koma muli ndi moyo, mukupanga zokupatsani ndalama mwaufulu posatengera zoipa za makolo anu. Mnyamatayu ndi waluso komwe ku Mangalande, akupititsa mbiri yabwino ya Malawi patsogolo. chommwe chiri chonyaditsa kwa wina aliyense. A Malawi tiyeni tisiye NSANJE!
Koma aChaponda dzina lokhalo silikuchititsani manyazi?
Are you not ashamed with your father to be a maize thief in a country of poor people.
Kansiime, can you make a joke about this fellow comedian of yours.