Email a copy of 'Dausi in ‘ivory-gate’ at Nyika National Park' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Dausi in ‘ivory-gate’ at Nyika National Park' to a friend
Human rights activist Billy Banda has advised opposition political parties, mainly Malawi Congress Party (MCP) to be more "constructive and...
You abuse our tax,you destroy our chikangawa and you are now butchering our elephants and you call yourselves leaders,all you think about is money,money,and money pali za integrity ndi patriotism apa?
dyera basi za ziiiii. muzingodikirana zaka 5 zikatha mulowa
Its good to do such business internationally why our nation Is poor. koma akanakhala munthu opanda dzina bwenzi mtammanga ndinu opusa
Ndikudabwanazo.Anthukwawokoakuti Simunthuwabwino Komamdziko Tikumuonakuti Alibwino.Akuwonetsa Wu Dausiwake
Izi sizodabwitsa ayi. Limeneli ndiye khalidwe la Dausi lenileni. Ife Dausi takhala naye ndiponso tagwila naye ntchito limodzi. Ngati anthu ankaponyedwa ndi kudyedwa ndi ng’ona nthawi ya Kamuzu, sidausi yemweyu? Dausi ankayika anthu mu zimatumba ndikuwaponya ku ng’ona.
Hahahahahahaha Koma Zili Ku Malawi Thuni Ayayayayaya
aah!!aah!!tsano apa muti mchiyaniso?mwagwidwa ni nyanga zo njovu yayi muluzisaka omalawi
My sister choose a man who is decent and humane,do not be attracted by wealth of somebody.This guy is among those who don’t care about the economic development in hinyaland,they would even be happier to destroy everything left in our region in order to leave Hinyaland a barren piece of land.Nyika National Park,is one of the best in the world,but it is located on the hated part of the country.Mind you I would not choose the husband for you,if I have hurted your feelings,I beg to apologies for that,but keep in mind that,our brothers and sisters from the South and… Read more »
No 21 Paka, woopa chiyani? Uja ananyamula ngona zinali ku MCP uja siemweyi?
Paka,woopa chiyani? munthu uja ananyamula ng’ona za ku MCP kupitisa ku DPP siemweyi?