Email a copy of 'After dumping Alliance, Chimbanga joins ruling DPP' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'After dumping Alliance, Chimbanga joins ruling DPP' to a friend
Lilongwe City South East by-election candidate for governing Democrtaic Progressive Party (DPP) Reuben Ngwenya has hired reggae artist Charles Nsaku...
National rebuilding exercise my foot! Just say you have received the 100 million rejected by Sitolo of Nsanje lalanje
Chimbanga contested the 2014 election as a UDF parliamentary candidate kwathu ku Dedza East koma adagwetsedwa ndi Juliana Lunguzi. I wish he had joined MCP kuti akalimbane internally ndi Juliana. He has a right to join any party koma I really wish he had joined MCP. Anyway, all the best, Leonard. Koma udzipita ku Ntakataka anthu adzikudziwa ngati ukufuna udzakhale MP wa Dedza East one day.
Political prostitute. Ndiye walawiliritu. No sane person can trust you Chimbanga.
Wabodza uyu…… studies have become DPP. Who, then, can trust him?
yes….. he wants to study for a Doctorate of Political Prostitution (DPP)
Akati munthu wachita misala ndiye za a Chimbanga’zi. Joining failures and looters of Malawi?
He has been a member of three political groupings in a space of 3 years, political prostitute in the making
Anamulumitsa chi bans
Akumudzi, ndinkadabwatu ine kuti mwatani ku panga ubale ndi munthu osowakwaoyi!!! Amati mkwakumangoni koma aaa , palibe!!! Adapha mwana wa chemwali pa ngozi ya galimoto kwa Kapesi and I will take him heard on!!!!