Email a copy of 'Eagles crowned 2018 Airtel Top 8 kings: End six-year cup drought' to a friend
Loading ...
Email a copy of 'Eagles crowned 2018 Airtel Top 8 kings: End six-year cup drought' to a friend
Former President Joyce Banda will be quizzed by government to establish the truth about the disposal of the French-made jet to...
Team yama savage iyi who do not always accept defeat . Akanakhala kuti penalty inali yao the blue eagles camp sakanavuta koma kuvomelza kuti koma si ma savage abullets. Chiukepo Msowoya must be banned from entering the football ground for life for his un sportsmanship behaviour no wonder samakhalitsa akapita kunja kokaswewera mpira. Mankhwala osewelera mpira sanagwire ntchito dzulo
I’m a Bullets supporter and was at Bingu Stadium to watch the Airtel Finals, let’s face facts, that was a genuine penalty and I was very disappointed to see Chiukepo leading in the attack of referees. Bullets players have aged and if nothing is done, we will not get anywhere.
Zitsilu, ma savage a bullets.
Awa ndiopoila akuyenela alandire zirango chifukwa aphwanya malamulo amumpira amaona ngati kuti iwowo nde ndakatakwe samavomeleza kuluza .tikufuna chilango chenicheni kuchokela kwa Chiukepo ndamzake atichitisa manyazi .dnt tek tym a fam nda sulom apa zithu zaipa tym ya ziwawa inatha.chomwe sanapite kukalandila ma medalz ndi chani entire comit aipanishe basi.